< Masalimo 61 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Loyimbidwa ndi zipangizo za zingwe. Imvani kulira kwanga, Inu Mulungu; mvetserani pemphero langa.
Rhotoeng neh aka mawt ham David kah Pathen aw ka tamlung he ya lamtah ka thangthuinah he hnatung lah.
2 Kuchokera ku malekezero a dziko lapansi ine ndimayitana Inu ndimayitana pomwe mtima wanga ukufowoka; tsogolereni ku thanthwe lalitali kuposa ineyo.
Nang te Diklai a bawt lamkah kan khue. Ka lungbuei a rhae vaengah kamah lakah aka sang lungpang taengla kai nan mawt.
3 Pakuti Inu mwakhala pothawirapo panga, nsanja yolimba polimbana ndi adani anga.
Kai ham tah hlipyingnah neh thunkha hmai ah sarhi rhaltoengim la na om.
4 Ine ndikulakalaka kukhala mʼtenti yanu kwamuyaya ndi kupeza chitetezo mu mthunzi wa mapiko anu.
Na dap khuiah kumhal ka bakuep vetih na phae hlip ah ka ying ni. (Selah)
5 Pakuti Inu Mulungu mwamva malumbiro anga; mwandipatsa cholowa cha iwo amene amaopa dzina lanu.
Pathen namah loh ka olcaeng te na yaak dongah na ming aka rhih tah rho na paek.
6 Wonjezerani masiku a moyo wa mfumu, zaka zake kwa mibado yochuluka.
Manghai kah a tue khohnin te puh sak lamtah a kum khaw cadilcahma duela nguel sak.
7 Iye akhale pa mpando waufumu pamaso pa Mulungu kwamuyaya; ikani chikondi chanu ndi kukhulupirika kwanu kuti zimuteteze.
Sitlohnah Pathen hmai ah kumhal khosa saeh lamtah a khueh oltak loh anih te kueinah saeh.
8 Kotero ndidzayimba matamando kwamuyaya pa dzina lanu ndi kukwaniritsa malumbiro anga tsiku ndi tsiku.
Khohnin, khohnin ah ka olcaeng te thuung ham na ming ka tingtoeng yoeyah.

< Masalimo 61 >