< Masalimo 6 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Molingana ndi seminiti. Salimo la Davide. Inu Yehova, musandidzudzule mu mkwiyo wanu, kapena kundilanga mu ukali wanu.
Kuom jatend wer. Miwero gi gig wer man-gi tondegi. Kaluwore gi sheminith. Zaburi Mar Daudi. Kik ikwera, yaye Jehova Nyasaye, ka iyi owangʼ kata kum kik ikuma ka mirima omaki.
2 Ndichitireni chifundo Inu Yehova, pakuti ndalefuka; Inu Yehova chiritseni, pakuti mafupa anga ali pa ululu waukulu.
Kecha, yaye Jehova Nyasaye, nikech aol; changa, yaye Jehova Nyasaye, nikech chokena rama malit.
3 Moyo wanga uli pa mazunzo aakulu. Mpaka liti, Inu Yehova, mpaka liti?
Chunya winjo malit. Nyaka karangʼo, yaye Jehova Nyasaye, nyaka karangʼo?
4 Tembenukani Inu Yehova, ndipo mundilanditse; pulumutseni chifukwa cha chikondi chanu chosasinthika.
Lokri, yaye Jehova Nyasaye, mondo iresa; resa nikech herani ma ok rum.
5 Palibe amene amakukumbukirani pamene wamwalira; Amakutamandani ndani ali ku manda? (Sheol h7585)
Onge ngʼama nyalo pari ka osetho. En ngʼa madi paki gi ei liel? (Sheol h7585)
6 Ine ndatopa ndi kubuwula; usiku wonse pa bedi panga pamadzaza ndi misozi yanga; ndimanyowetsa pogona panga ndi misozi.
Chur ma achurgo ojonya otieno duto abudo kitandana gi ywak, kendo pi wangʼa olwoko piendena.
7 Maso anga atupa chifukwa cha chisoni; akulephera kuona chifukwa cha adani anga.
Wengena ool nikech lit ma an-go; ok ginen maber nikech wasika duto.
8 Chokani kwa ine inu nonse amene mumachita zoyipa, pakuti Yehova wamva kulira kwanga.
Ayiuru buta, un duto ji matimo richo, nikech Jehova Nyasaye osewinjo ywakna.
9 Yehova wamva kupempha kwanga kofuna chifundo; Yehova walandira pemphero langa.
Jehova Nyasaye osewinjo ywak mar kwayo kech; Jehova Nyasaye orwako lamo mara.
10 Adani anga onse adzachita manyazi ndipo adzakhala ndi mantha; adzabwerera msangamsanga mwa manyazi.
Wasika duto wigi biro kuot kendo gibiro hum nono; gibiro dok chien apoya nono gi wichkuot.

< Masalimo 6 >