< Masalimo 59 >
1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Musawononge.” Ndakatulo ya Davide. Pamene Sauli anatumiza anthu kuti akalondere nyumba ya Davide ndi cholinga choti amuphe. Landitseni kwa adani anga, Inu Mulungu; munditeteze kwa anthu amene auka kutsutsana nane.
Aka mawt ham, Saul loh a tueih tih ngawn ham im ah a tawt uh vaengkah David kah Phae Boeh laa Ka Pathen aw ka thunkha rhoek kut lamkah kai n'huul lah. Kai aka tlai thil rhoek kut lamkah kai n'hoeptlang lah.
2 Landitseni kwa anthu ochita zoyipa ndipo mundipulumutse kwa anthu okhetsa magazi.
Boethae aka saii rhoek kut lamkah kai n'huul lamtah hlang thii aka haal rhoek kut lamkah kai n'khang lah.
3 Onani momwe iwo akundibisalira! Anthu owopsa agwirizana zolimbana nane; osati chifukwa cha mlandu kapena tchimo langa, Inu Yehova.
Ka hinglu te a rhongngol thil uh coeng ke. Ka boekoek khaw om pawt tih BOEIPA ka tholhnah khaw om pawt dae hlangtlung rhoek loh kai m'mae uh.
4 Ine sindinachite cholakwa, koma iwo ndi okonzeka kundithira nkhondo. Dzukani kuti mundithandize; penyani mavuto anga!
Thaesainah om pawt dae ha yong uh tih tawn uh. Kai aka doe ham long tah haenghang lamtah hmuh lah.
5 Inu Yehova Mulungu Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli, dzidzutseni nokha kuti mulange anthu a mitundu ina yonse; musaonetse chifundo chanu kwa anthu oyipa achinyengowa.
Te dongah namtom boeih te cawh hamla, caempuei Pathen, BOEIPA, Israel Pathen namah mah thoo lamtah boethae neh aka hnukpoh boeih te rhen boeh. (Selah)
6 Iwo amabweranso madzulo akuchita phokoso ngati agalu ndi kumangoyendayenda mu mzinda.
Hlaemhmah ah amih loh ha mael uh tih ui bangla a phit uh doel a khopuei a hil uh.
7 Onani zomwe amalavula mʼkamwa mwawo; iwo amalavula malupanga kuchokera pa milomo yawo, ndipo amanena kuti, “Ndani angatimve?”
A hmui kah cunghang ke, “Unim aka ya,” tila a ka lamkah ol te a thaa uh van ke?
8 Koma Inu Yehova, mumawaseka, mumayinyoza mitundu yonseyo.
Tedae BOEIPA nang loh amih te na nueih thil tih namtom boeih ke na tamdaeng.
9 Inu mphamvu yanga, ine ndiyangʼana kwa inu; Inu Mulungu, ndinu linga langa.
Anih kah sarhi vanbangla, Pathen khaw kai ham imsang la a om dongah namah ni kan rhingda.
10 Mulungu wanga wachikondi. Mulungu adzapita patsogolo panga ndipo adzandilola kunyada pa iwo amene amandinyoza.
Kai ham sitlohnah kah sitlohnah Pathen loh kai n'doe ni. Ka lungawn rhoek soah Pathen loh kai n'sawt sak ni.
11 Koma musawaphe, Inu Ambuye chishango chathu, kuopa kuti anthu anga angayiwale. Mwa mphamvu zanu, lolani kuti azingoyendayenda ndipo muwatsitse.
Amih te ngawn boel mai, ka pilnam te hnilh ve. Ka Boeipa, kaimih kah photling aw, na thadueng neh amih te poengdoe sak lamtah suntlak sak.
12 Chifukwa cha machimo a pakamwa pawo chifukwa cha mawu a milomo yawo, iwo akodwe mʼkunyada kwawo. Chifukwa cha matemberero ndi mabodza amene ayankhula
Thaephoeinah neh laithae a doek uh dongah amamih ka kah tholhnah, amamih hmui kah olka neh amamih kah hoemdamnah dongah man uh saeh.
13 muwawononge mu ukali (wanu) muwawononge mpaka atheretu. Pamenepo zidzadziwika ku malekezero a dziko lapansi kuti Mulungu amalamulira Yakobo.
Amih te kosi dongah muei muei tih a milh daengah ni Jakob neh diklai a bawt duela aka taemrhai he Pathen ni tila aming uh eh. (Selah)
14 Iwo amabweranso madzulo, akuchita phokoso ngati agalu ndi kumangoyenda mu mzinda.
Hlaemhmah ah ha mael uh bal saeh lamtah ui bangla a phit uh doel a khopuei hil uh bal saeh.
15 Iwo amayendayenda kufuna chakudya ndipo amawuwa ngati sanakhute.
Amih loh buhtuen la poeng poeng uh tih a hah uh pawt vaengah rhaehba uh sut.
16 Koma ine ndidzayimba za mphamvu yanu, mmawa ndidzayimba zachikondi chanu; pakuti ndinu linga langa, pothawirapo panga mʼnthawi ya mavuto.
Tedae kai tah, na sarhi te ka hlai vetih, namah te kai ham imsang neh kai taengkah puencak tue vaengah thuhaelnah la na om dongah, na sitlohnah khaw mincang ah ka tamhoe puei ni.
17 Inu mphamvu yanga, ndiyimba matamando kwa inu; Inu Mulungu, ndinu linga langa, Mulungu wanga wachikondi.
Ka sitlohnah Pathen neh ka imsang Pathen ham tah nang taengah ka sarhi ka tingtoeng.