< Masalimo 54 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Ndakatulo ya Davide. Pamene anthu a ku Zifi anapita kwa Sauli ndipo anati, “Kodi Davide sakubisala pakati pathu.” Pulumutseni Inu Mulungu, mwa dzina lanu; onetsani kuti ndine wosalakwa mwamphamvu yanu.
En undervisning Davids, till att föresjunga på strängaspel; Då de af Siph kommo, och sade till Saul: David hafver fördolt sig när oss. Hjelp mig, Gud, genom ditt Namn, och skaffa mig rätt genom dina magt.
2 Imvani pemphero langa, Inu Mulungu mvetserani mawu a pakamwa panga.
Gud, hör min bön; förnim mins muns tal.
3 Alendo akundithira nkhondo; anthu ankhanza akufunafuna moyo wanga, anthu amene salabadira za Mulungu.
Ty stolte sätta sig emot mig, och våldsverkare stå efter mina själ; och hafva intet Gud för ögon. (Sela)
4 Zoonadi Mulungu ndi thandizo langa; Ambuye ndiye amene amandichirikiza ine.
Si, Gud står med mig; Herren uppehåller mina själ.
5 Lolani kuti choyipa chifike pa iwo amene amandichita chipongwe; mwa kukhulupirika kwanu awonongeni.
Han skall betala minom fiendom det onda; förstör dem genom dina trohet;
6 Ine ndidzapereka nsembe yaufulu kwa Inu; ndidzatamanda dzina lanu, Inu Yehova, pakuti ndi labwino.
Så vill jag göra dig ett glädjeoffer, och tacka, Herre, dino Namne, att det så trösteligit är.
7 Pakuti Iyeyo wandipulumutsa ku masautso anga onse, ndipo maso anga apenya kupambana kwa pa adani anga.
Ty du hjelper mig utur all min nöd, att mina ögon måga på mina fiendar lust se.

< Masalimo 54 >