< Masalimo 54 >
1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Ndakatulo ya Davide. Pamene anthu a ku Zifi anapita kwa Sauli ndipo anati, “Kodi Davide sakubisala pakati pathu.” Pulumutseni Inu Mulungu, mwa dzina lanu; onetsani kuti ndine wosalakwa mwamphamvu yanu.
Rombaho iraho ry Andrianañahare ty amy tahina’oy, vaho meo-to amo haozara’oo.
2 Imvani pemphero langa, Inu Mulungu mvetserani mawu a pakamwa panga.
Ry Andrianañahare, janjiño ty halaliko, toloro ravembia o entam-bavakoo.
3 Alendo akundithira nkhondo; anthu ankhanza akufunafuna moyo wanga, anthu amene salabadira za Mulungu.
Miongake hiatreatre ahy ty ambahiny, paia’ o mitrotrofiakeo ty fiaiko, tsy nampiaoloe’ iareo t’i Andrianañahare. Selà
4 Zoonadi Mulungu ndi thandizo langa; Ambuye ndiye amene amandichirikiza ine.
Inao! Mpañimb’ahy t’i Andrianañahare, Fiatoam-piaiko t’i Talè.
5 Lolani kuti choyipa chifike pa iwo amene amandichita chipongwe; mwa kukhulupirika kwanu awonongeni.
Hafote’e amo mivoñoñe ahiko ty haratia’ iareo; Rotsaho iereo ami’ty figahiña’o.
6 Ine ndidzapereka nsembe yaufulu kwa Inu; ndidzatamanda dzina lanu, Inu Yehova, pakuti ndi labwino.
Mañenga ama’o an-tsatrin-tro iraho, andriañeko i tahina’oy ry Iehovà, amy te ie ty soa;
7 Pakuti Iyeyo wandipulumutsa ku masautso anga onse, ndipo maso anga apenya kupambana kwa pa adani anga.
Fa nafaha’e amako ze hene haemberañe, vaho nisambae’ o masokoo o rafelahikoo.