< Masalimo 54 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Ndakatulo ya Davide. Pamene anthu a ku Zifi anapita kwa Sauli ndipo anati, “Kodi Davide sakubisala pakati pathu.” Pulumutseni Inu Mulungu, mwa dzina lanu; onetsani kuti ndine wosalakwa mwamphamvu yanu.
Luwasa ako, O Dios, pinaagi sa imong ngalan, ug hukmi ako sa imong kusog.
2 Imvani pemphero langa, Inu Mulungu mvetserani mawu a pakamwa panga.
Dungga ang akong pag-ampo, Dios; paminawa ang mga pulong sa akong baba.
3 Alendo akundithira nkhondo; anthu ankhanza akufunafuna moyo wanga, anthu amene salabadira za Mulungu.
Kay ang mga langyaw nakigbatok kanako, ug ang mga walay kaluoy nga kalalakin-an nangita sa akong kinabuhi. Wala nila gibutang ang Dios taliwala kanila. (Selah)
4 Zoonadi Mulungu ndi thandizo langa; Ambuye ndiye amene amandichirikiza ine.
Tan-awa, ang Dios maoy akong magtatabang, ang Ginoo maoy naglaban kanako.
5 Lolani kuti choyipa chifike pa iwo amene amandichita chipongwe; mwa kukhulupirika kwanu awonongeni.
Panimaslan niya ug daotan ang akong mga kaaway; sa imong pagkamatinud-anon, laglaga (sila)
6 Ine ndidzapereka nsembe yaufulu kwa Inu; ndidzatamanda dzina lanu, Inu Yehova, pakuti ndi labwino.
Magahalad ako kanimo ug kinabubut-ong halad; magpasalamat ako sa imong ngalan, Yahweh, tungod kay maayo kini.
7 Pakuti Iyeyo wandipulumutsa ku masautso anga onse, ndipo maso anga apenya kupambana kwa pa adani anga.
Kay giluwas niya ako sa tanang pagsulay; ang akong mata nagtan-aw sa kadaogan ngadto sa akong mga kaaway.

< Masalimo 54 >