< Masalimo 53 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a Mahalati. Ndakatulo ya Davide. Chitsiru chimati mu mtima mwake, “Kulibe Mulungu.” Iwo ndi oyipa ndipo njira zawo ndi zonyansa; palibe ndi mmodzi yemwe amene amachita chabwino.
Davidin opetus, edelläveisaajalle, Mahelatin päällä. Tyhmät sanovat sydämessänsä: ei Jumalaa olekaan; ei he mitään kelpaa, ja ovat ilkiät menoissansa: ei ole joka hyvää tekee.
2 Mulungu kumwamba amayangʼana pansi pano pa ana a anthu kuti aone ngati alipo wina wanzeru, wofunafuna Mulungu.
Jumala katsoi taivaasta ihmisten lapsia, nähdäksensä, jos joku ymmärtäis, joku Jumalaa etsis.
3 Aliyense wabwerera, iwo onse pamodzi akhala oyipa; palibe ndi mmodzi yemwe amene amachita chabwino, ngakhale mmodzi.
Mutta he ovat kaikki vilpistelleet, ja kaikki ovat kelvottomiksi tulleet: ei ole yksikään, joka hyvää tekee, ei ainoakaan.
4 Kodi anthu ochita zoyipawa adzaphunziradi; anthu amene amadya anthu anga monga mmene anthu amadyera buledi, ndipo sapemphera kwa Mulungu?
Eivätkö pahantekiät sitä huomaitse? jotka minun kansaani syövät, niinkuin he söisivät leipää; vaan ei he Jumalaa avuksensa huuda.
5 Iwo anali pamenepo atathedwa nzeru ndi mantha aakulu pamene panalibe kanthu kochititsa mantha. Mulungu anamwazamwaza mafupa a anthu amene anakuthirani nkhondo; inuyo munawachititsa manyazi, pakuti Mulungu anawanyoza.
Siellä he kovin pelkäsivät, kussa ei mitään peljättävää ollut; sillä Jumala hajoittaa niiden luut, jotka sinua ahdistavat: sinä saatat heitä häpiään, sillä Jumala hylkää heidät.
6 Ndithu, chipulumutso cha Israeli nʼchochokera ku Ziyoni! Pamene Mulungu adzabwezeretsanso ulemerero wa anthu ake, lolani Yakobo akondwere ndi Israeli asangalale!
Oi, jos apu tulis Zionista Israelille! Kuin Jumala vangitun kansansa päästää, niin Jakob iloitsee ja Israel riemuitsee.

< Masalimo 53 >