< Masalimo 52 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe, ndakatulo ya Davide; pamene Doegi Mwedomu anapita kwa Sauli ndi kunena kuti “Davide wapita ku nyumba ya Ahimeleki.” Nʼchifukwa chiyani ukudzitamandira ndi zoyipa, iwe munthu wamphamvu? Nʼchifukwa chiyani ukudzitamandira tsiku lonse, iwe munthu wochititsa manyazi pamaso pa Mulungu?
Davidin opetus, edelläveisaajalle, Kuin Edomilainen Doeg tuli ja ilmoitti Saulille, ja sanoi hänelle: David on tullut Ahimelekin huoneeseen. Mitäs kerskaat pahuudessas, sinä väkevä? Jumalan laupius pysyy joka päivä.
2 Tsiku lonse umakhalira kuganizira za kuwononga ena; lilime lako lili ngati lumo lakuthwa, ntchito yako nʼkunyenga.
Sinun kieles ajattelee vahinkoa ja leikkaa valheellansa niinkuin terävä partaveitsi.
3 Iwe umakonda choyipa mʼmalo mwa kuyankhula choonadi. Umakonda kunama kupambana kuyankhula zoona. (Sela)
Sinä rakastat enempi pahaa kuin hyvää, ja puhut valhetta pikemmin kuin oikeutta, (Sela)
4 Umakonda mawu onse opweteka, iwe lilime lachinyengo!
Sinä puhut mielelläs kaikkia murhasanoja väärällä kielellä.
5 Zoonadi Mulungu adzakutsitsa kupita ku chiwonongeko chamuyaya: iye adzakukwatula ndi kukuchotsa mʼtenti yako; iye adzakuzula kuchoka mʼdziko la amoyo.
Niin Jumala myös kukistaa sinun ijankaikkisesti: hän murentaa sinun, ja majasta tempaa sinun ulos, ja juurittaa sinun ulos eläväin maalta, (Sela)
6 Olungama adzaona zimenezi ndi kuchita mantha; adzamuseka nʼkumanena kuti,
Ja vanhurskasten pitää sen näkemän ja pelkäämän; ja he nauravat häntä.
7 “Pano tsopano pali munthu amene sanayese Mulungu linga lake, koma anakhulupirira chuma chake chambiri nalimbika kuchita zoyipa!”
Katso, tämä on se mies, joka ei pitänyt Jumalaa turvanansa, vaan uskalsi suureen rikkauteensa: hän on vahvistunut pahuudessansa.
8 Koma ine ndili ngati mtengo wa olivi wobiriwira bwino mʼnyumba ya Mulungu; ndimadalira chikondi chosatha cha Mulungu kwa nthawi za nthawi.
Mutta minä olen niinkuin viheriäinen öljypuu Herran huoneessa: minä uskallan Jumalan laupiuteen aina ja ijankaikkisesti.
9 Ine ndidzakutamandani kwamuyaya chifukwa cha zimene mwachita; chifukwa cha zimene mwachita; mʼdzina lanu ndidzayembekezera pakuti dzina lanulo ndi labwino. Ndidzakutamandani pamaso pa oyera mtima anu.
Minä tahdon sinua kiittää ijankaikkisesti, ettäs sen teit, ja odottaa sinun nimeäs; sillä se on hyvä sinun pyhäis edessä.

< Masalimo 52 >