< Masalimo 51 >
1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Pamene Mneneri Natani anabwera kwa iye atachita chigololo ndi Batiseba. Mundichitire chifundo, Inu Mulungu, molingana ndi chikondi chanu chosasinthika; molingana ndi chifundo chanu chachikulu mufafanize mphulupulu zanga.
Ай милэ де мине, Думнезеуле, ын бунэтатя Та! Дупэ ындураря Та чя маре, штерӂе фэрэделеӂиле меле!
2 Munditsuke zolakwa zanga zonse ndipo mundiyeretse kuchotsa tchimo langa.
Спалэ-мэ ку десэвыршире де нелеӂюиря мя ши курэцеште-мэ де пэкатул меу!
3 Pakuti ndikudziwa mphulupulu zanga, ndipo tchimo langa lili pamaso panga nthawi zonse.
Кэч ымь куноск бине фэрэделеӂиле ши пэкатул меу стэ некурмат ынаинтя мя.
4 Motsutsana ndi Inu, Inu nokha, ndachimwa ndipo ndachita zoyipa pamaso panu, Kotero kuti inu mwapezeka kuti ndinu wolungama pamene muyankhula ndi pamene muweruza.
Ымпотрива Та, нумай ымпотрива Та ам пэкэтуит ши ам фэкут че есте рэу ынаинтя Та; аша кэ вей фи дрепт ын хотэрыря Та ши фэрэ винэ ын жудеката Та.
5 Zoonadi ine ndinali wochimwa pomwe ndimabadwa, wochimwa kuyambira pa nthawi imene amayi anga anakhala woyembekezera ine.
Ятэ кэ сунт нэскут ын нелеӂюире ши ын пэкат м-а зэмислит мама мя.
6 Zoonadi inu mumafuna choonadi mu ziwalo zamʼkati mwanga; mumandiphunzitsa nzeru mʼkati mwanga mwenimweni.
Дар Ту черь ка адевэрул сэ фие ын адынкул инимий: фэ дар сэ пэтрундэ ынцелепчуня ынэунтрул меу!
7 Mundiyeretse ndi hisope ndipo ndidzayera, munditsuke ndipo ndidzayera kuposa matalala
Курэцеште-мэ ку исоп ши вой фи курат; спалэ-мэ ши вой фи май алб декыт зэпада!
8 Mundilole ndimve chimwemwe ndi chisangalalo, mulole kuti mafupa amene mwawamphwanya akondwere.
Фэ-мэ сэ ауд веселие ши букурие ши оаселе пе каре ле-ай здробит Ту се вор букура!
9 Mufulatire machimo anga ndi kufafaniza zolakwa zanga zonse.
Ынтоарче-Ць привиря де ла пэкателе меле, штерӂе тоате нелеӂюириле меле!
10 Mulenge mʼkati mwanga mtima woyera Inu Mulungu ndi kukonzanso mzimu wokhazikika mwa ine.
Зидеште ын мине о инимэ куратэ, Думнезеуле, пуне ын мине ун дух ноу ши статорник!
11 Musandichotse pamaso panu kapena kuchotsa Mzimu wanu Woyera mwa ine.
Ну мэ лепэда де ла Фаца Та ши ну луа де ла мине Духул Тэу чел Сфынт!
12 Bwezeretsani mwa ine chimwemwe cha chipulumutso chanu ndipo mundipatse mzimu wofuna kumvera kuti undilimbitse.
Дэ-мь ярэшь букурия мынтуирий Тале ши сприжинэ-мэ ку ун дух де бунэвоинцэ!
13 Pamenepo ndidzaphunzitsa anthu amphulupulu njira zanu kuti ochimwa adzabwerere kwa inu.
Атунч вой ынвэца кэиле Тале пе чей че ле калкэ, ши пэкэтоший се вор ынтоарче ла Тине.
14 Mundipulumutse ku tchimo lokhetsa magazi, Inu Mulungu, Mulungu wa chipulumutso changa, ndipo lilime langa lidzayimba zachilungamo chanu.
Думнезеуле, Думнезеул мынтуирий меле! Избэвеште-мэ де вина сынӂелуй вэрсат ши лимба мя ва лэуда ындураря Та!
15 Inu Ambuye tsekulani milomo yanga, ndipo pakamwa panga padzalengeza matamando anu.
Доамне, дескиде-мь бузеле ши гура мя ва вести лауда Та!
16 Inu simusangalatsidwa ndi nsembe wamba. Ndikanapereka nsembe yopsereza, Inu simukondwera nayo.
Дакэ ай фи воит жертфе, Ць-аш фи адус, дар Цие ну-Ць плак ардериле-де-тот.
17 Nsembe za Mulungu ndi mzimu wosweka; mtima wosweka ndi wachisoni Inu Mulungu simudzawunyoza.
Жертфеле плэкуте луй Думнезеу сунт ун дух здробит: Думнезеуле, Ту ну диспрецуешть о инимэ здробитэ ши мыхнитэ.
18 Mwa kukoma mtima kwanu mupange Ziyoni kuti alemere; mumange makoma a Yerusalemu.
Ын ындураря Та, варсэ-Ць бинефачериле асупра Сионулуй ши зидеште зидуриле Иерусалимулуй!
19 Kotero kudzakhala nsembe zachilungamo, nsembe yonse yopsereza yokondweretsa Inu; ndipo ngʼombe zazimuna zidzaperekedwa pa guwa lanu la nsembe.
Атунч вей прими жертфе неприхэните, ардерь-де-тот ши жертфе ынтреӂь; атунч се вор адуче пе алтарул Тэу вицей.