< Masalimo 51 >
1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Pamene Mneneri Natani anabwera kwa iye atachita chigololo ndi Batiseba. Mundichitire chifundo, Inu Mulungu, molingana ndi chikondi chanu chosasinthika; molingana ndi chifundo chanu chachikulu mufafanize mphulupulu zanga.
Til Sangmesteren; en Psalme af David,
2 Munditsuke zolakwa zanga zonse ndipo mundiyeretse kuchotsa tchimo langa.
der Profeten Nathan var kommen til ham, efter at han var gaaet ind til Bathseba.
3 Pakuti ndikudziwa mphulupulu zanga, ndipo tchimo langa lili pamaso panga nthawi zonse.
Gud! vær mig naadig efter din Miskundhed, udslet mine Overtrædelser efter din store Barmhjertighed.
4 Motsutsana ndi Inu, Inu nokha, ndachimwa ndipo ndachita zoyipa pamaso panu, Kotero kuti inu mwapezeka kuti ndinu wolungama pamene muyankhula ndi pamene muweruza.
To mig vel af min Misgerning og rens mig Ira min Synd;
5 Zoonadi ine ndinali wochimwa pomwe ndimabadwa, wochimwa kuyambira pa nthawi imene amayi anga anakhala woyembekezera ine.
thi mine Overtrædelser kender jeg, og min Synd er altid for mig.
6 Zoonadi inu mumafuna choonadi mu ziwalo zamʼkati mwanga; mumandiphunzitsa nzeru mʼkati mwanga mwenimweni.
Imod dig, imod dig alene har jeg syndet og gjort det onde for dine Øjne, paa det du skal være retfærdig, naar du taler, være ren, naar du dømmer.
7 Mundiyeretse ndi hisope ndipo ndidzayera, munditsuke ndipo ndidzayera kuposa matalala
Se, jeg er født i Skyld, og min Moder har undfanget mig i Synd.
8 Mundilole ndimve chimwemwe ndi chisangalalo, mulole kuti mafupa amene mwawamphwanya akondwere.
Se, til Sandhed i det inderste Hjerte har du Lyst; Visdommen i Hjertedybet lære du mig!
9 Mufulatire machimo anga ndi kufafaniza zolakwa zanga zonse.
Rens mig fra Synd med Isop, saa jeg bliver ren; to mig, saa jeg bliver hvidere end Sne.
10 Mulenge mʼkati mwanga mtima woyera Inu Mulungu ndi kukonzanso mzimu wokhazikika mwa ine.
Lad mig høre Fryd og Glæde; lad de Ben fryde sig, som du har sønderstødt.
11 Musandichotse pamaso panu kapena kuchotsa Mzimu wanu Woyera mwa ine.
Skjul dit Ansigt for mine Synder og udslet alle mine Misgerninger!
12 Bwezeretsani mwa ine chimwemwe cha chipulumutso chanu ndipo mundipatse mzimu wofuna kumvera kuti undilimbitse.
Gud! skab mig et rent Hjerte og forny en stadig Aand inden i mig.
13 Pamenepo ndidzaphunzitsa anthu amphulupulu njira zanu kuti ochimwa adzabwerere kwa inu.
Bortkast mig ikke fra dit Ansigt og tag ikke din Helligaand fra mig!
14 Mundipulumutse ku tchimo lokhetsa magazi, Inu Mulungu, Mulungu wa chipulumutso changa, ndipo lilime langa lidzayimba zachilungamo chanu.
Giv mig igen at glædes over din Frelse og ophold mig med en villig Aand!
15 Inu Ambuye tsekulani milomo yanga, ndipo pakamwa panga padzalengeza matamando anu.
Saa vil jeg lære Overtrædere dine Veje, og Syndere skulle omvende sig til dig.
16 Inu simusangalatsidwa ndi nsembe wamba. Ndikanapereka nsembe yopsereza, Inu simukondwera nayo.
Fri mig fra Blodskyld, Gud, min Frelses Gud! saa skal min Tunge synge med Fryd om din Retfærdighed.
17 Nsembe za Mulungu ndi mzimu wosweka; mtima wosweka ndi wachisoni Inu Mulungu simudzawunyoza.
Herre! oplad mine Læber, saa skal min Mund kundgøre din Pris.
18 Mwa kukoma mtima kwanu mupange Ziyoni kuti alemere; mumange makoma a Yerusalemu.
Thi du har ikke Lyst til Slagtoffer, ellers vilde jeg give dig det; til Brændoffer har du ikke Behagelighed.
19 Kotero kudzakhala nsembe zachilungamo, nsembe yonse yopsereza yokondweretsa Inu; ndipo ngʼombe zazimuna zidzaperekedwa pa guwa lanu la nsembe.
Ofre for Gud er en sønderbrudt Aand; et sønderbrudt og sønderstødt Hjerte skal du, o Gud! ikke foragte. Gør vel imod Zion efter din Velbehagelighed, byg Jerusalems Mure, da vil du have Lyst til Retfærdigheds Ofre, Brændofre og Helofre; da skulle de ofre Øksne paa dit Alter.