< Masalimo 51 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Pamene Mneneri Natani anabwera kwa iye atachita chigololo ndi Batiseba. Mundichitire chifundo, Inu Mulungu, molingana ndi chikondi chanu chosasinthika; molingana ndi chifundo chanu chachikulu mufafanize mphulupulu zanga.
Aka mawt ham, Bathsheba taengla a caeh vanbangla tonghma Nathan loh anih a paan vaengkah David tingtoenglung Pathen aw kai n'rhen lah. Na sitlohnah neh na haidamnah a cungkuem vanbangla ka boekoeknah he han huih mai.
2 Munditsuke zolakwa zanga zonse ndipo mundiyeretse kuchotsa tchimo langa.
Kai kathaesainah loh a yet khaw a yet oeh dongah kai n'sil lamtah ka tholhnah lamkah kai n'caihcil lah.
3 Pakuti ndikudziwa mphulupulu zanga, ndipo tchimo langa lili pamaso panga nthawi zonse.
Kamah kah boekoek te kamah loh ka ming tih ka tholhnah loh kamah hmaiah om taitu.
4 Motsutsana ndi Inu, Inu nokha, ndachimwa ndipo ndachita zoyipa pamaso panu, Kotero kuti inu mwapezeka kuti ndinu wolungama pamene muyankhula ndi pamene muweruza.
Nang namah bueng taengah ka tholh tih na mikhmuh ah boethae ka saii. Tedae na thui vaengah nan tang sak tih nan cawh vaengah nan cim sak.
5 Zoonadi ine ndinali wochimwa pomwe ndimabadwa, wochimwa kuyambira pa nthawi imene amayi anga anakhala woyembekezera ine.
Thaesainah neh ka thang tih tholhnah neh a nu loh kai n'yom.
6 Zoonadi inu mumafuna choonadi mu ziwalo zamʼkati mwanga; mumandiphunzitsa nzeru mʼkati mwanga mwenimweni.
Kodang khuikah oltak te na ngaih dongah cueihnah na kael neh kai nan tuk nan kil.
7 Mundiyeretse ndi hisope ndipo ndidzayera, munditsuke ndipo ndidzayera kuposa matalala
Pumpiding neh kai nan cil daengah ni ka caihcil eh. Kai nan silh daengah ni vuelsong lakah ka bok eh.
8 Mundilole ndimve chimwemwe ndi chisangalalo, mulole kuti mafupa amene mwawamphwanya akondwere.
Omngaihnah neh kohoenah te kai nan yaak sak dongah na khaem tangtae rhuhrhong long khaw omngaih uh saeh.
9 Mufulatire machimo anga ndi kufafaniza zolakwa zanga zonse.
Ka tholhnah dongah na maelhmai thuh mai lamtah ka thaesainah boeih he han huih lah.
10 Mulenge mʼkati mwanga mtima woyera Inu Mulungu ndi kukonzanso mzimu wokhazikika mwa ine.
Pathen aw kai ham aka caih lungbuei han suen lamtah ka khui kah mueihla he cikngae la pan han tlaih lah.
11 Musandichotse pamaso panu kapena kuchotsa Mzimu wanu Woyera mwa ine.
Kai he namah mikhmuh lamkah m'voei boel lamtah kai taengkah Mueihla Cim lo boel mai.
12 Bwezeretsani mwa ine chimwemwe cha chipulumutso chanu ndipo mundipatse mzimu wofuna kumvera kuti undilimbitse.
Na daemnah, omngaihnah te kai taengah ha mael lamtah, moeihoeihnah mueihla loh kai n'talong saeh.
13 Pamenepo ndidzaphunzitsa anthu amphulupulu njira zanu kuti ochimwa adzabwerere kwa inu.
Boekoek rhoek te na khosing ka cang puei vetih hlangtholh rhoek loh nang taengla ha bal uh bitni.
14 Mundipulumutse ku tchimo lokhetsa magazi, Inu Mulungu, Mulungu wa chipulumutso changa, ndipo lilime langa lidzayimba zachilungamo chanu.
Pathen, ka loeihnah Pathen hlang thii lamkah kai n'huul lah. Nang kah duengnah te ka lai loh tamhoe puei saeh.
15 Inu Ambuye tsekulani milomo yanga, ndipo pakamwa panga padzalengeza matamando anu.
Ka Boeipa aw, ka hmui he han ong lamtah ka ka loh nang koehnah te doek saeh.
16 Inu simusangalatsidwa ndi nsembe wamba. Ndikanapereka nsembe yopsereza, Inu simukondwera nayo.
Hmueih he na ngaih pawt dongah ni na ngaih koinih kam paek mai sue. Hmueihhlutnah khaw na doe moenih.
17 Nsembe za Mulungu ndi mzimu wosweka; mtima wosweka ndi wachisoni Inu Mulungu simudzawunyoza.
Pathen kah a ngaih hmueih tah mueihla aka paeng ke ni. Lungbuei aka paeng tih aka paep te Pathen nang loh na hnawt moenih.
18 Mwa kukoma mtima kwanu mupange Ziyoni kuti alemere; mumange makoma a Yerusalemu.
Namah kah kolonah dongah Zion te khophoeng pha sak lamtah Jerusalem vongtung te khueng pah.
19 Kotero kudzakhala nsembe zachilungamo, nsembe yonse yopsereza yokondweretsa Inu; ndipo ngʼombe zazimuna zidzaperekedwa pa guwa lanu la nsembe.
Te vaengah, duengnah hmueih, hmueihhlutnah khaw boeih na ngaih vetih na hmueihtuk ah vaito a khuen uh ni.

< Masalimo 51 >