< Masalimo 50 >

1 Salimo la Asafu. Wamphamvuyo, Yehova Mulungu, akuyankhula ndi kuyitanitsa dziko lapansi kuyambira kotulukira dzuwa mpaka kumene limalowera.
Ihubo lika-Asafi. USomandla, uNkulunkulu, uThixo, uyakhuluma, ubiza umhlaba kusukela okuphuma khona ilanga kuze kufike lapho elitshona khona.
2 Kuchokera ku Ziyoni, mokongola kwambiri Mulungu akuwala.
EseZiyoni, epheleleyo ngobuhle, uNkulunkulu uyakhazimula.
3 Mulungu wathu akubwera ndipo sadzakhala chete; moto ukunyeketsa patsogolo pake, ndipo pomuzungulira pali mphepo yamkuntho
UNkulunkulu wethu uyeza, kayikuthula; umlilo uyahangula phambi kwakhe, emaceleni akhe kukhukhula isiphepho.
4 Iye akuyitanitsa zamumlengalenga ndi za pa dziko lapansi kuti aweruze anthu ake.
Ubiza amazulu ngaphezulu lomhlaba, ukuze ehlulele abantu bakhe:
5 Mundisonkhanitsire okhulupirika anga, amene anachita pangano ndi ine pochita nsembe.
“Qoqani kimi abahlanjululiweyo bami, abenza isivumelwano lami ngemihlatshelo.”
6 Ndipo mayiko akumwamba akulengeza chilungamo chake, pakuti Mulungu mwini ndi woweruza.
Lamazulu atshumayela ukulunga kwakhe; ngoba uNkulunkulu ngumahluleli ngokwakhe.
7 Imvani inu anthu anga, ndipo Ine ndidzayankhula, iwe Israeli, ndipo Ine ndidzayankhula mokutsutsa; ndine Mulungu, Mulungu wako.
“Zwanini, bantu bami, ngizakhuluma; yebo Israyeli, ngizafakaza ngimelane lawe; nginguNkulunkulu, Nkulunkulu wakho
8 Sindikudzudzula chifukwa cha nsembe zako, kapena nsembe zako zopsereza zimene zili pamaso panga nthawi zonse.
Kangikukhuzi ngemihlatshelo yakho kumbe iminikelo yakho yokutshiswa, ehlezi ikhona phambi kwami.
9 Ine sindikufuna ngʼombe yayimuna kuchokera mʼkhola lako kapena mbuzi za mʼkhola lako,
Angisweli inkunzi ephuma esibayeni sakho kumbe imbuzi zesilugu sakho,
10 pakuti nyama iliyonse yakunkhalango ndi yanga ndiponso ngʼombe za ku mapiri ochuluka.
ngoba yiphi layiphi inyamazana yeganga ngeyami, lenkomo ezisemaqaqeni azinkulungwane.
11 Ine ndimadziwa mbalame iliyonse mʼmapiri ndiponso zolengedwa zonse zakutchire ndi zanga.
Ngazi zonke izinyoni ezisezintabeni, lezidalwa zeganga ngezami.
12 Ndikanakhala ndi njala sindikanakuwuzani, pakuti dziko lonse ndi zonse zimene zili mʼmenemo ndi zanga.
Aluba ngangingolambayo ngangingekulitshela, ngoba umhlaba ngowami, lakho konke okukuwo.
13 Kodi ndimadya nyama ya ngʼombe zazimuna kapena kumwa magazi a mbuzi?
Ngidla inyama yezinkunzi yini kumbe nginatha igazi lembuzi na?
14 “Pereka nsembe zachiyamiko kwa Mulungu, kwaniritsa malonjezo ako kwa Wammwambamwamba.
Yenzani imihlatshelo yokubonga kuNkulunkulu, gcwalisani izifungo zenu koPhezukonke,
15 Ndipo undiyitane pa tsiku lako la masautso; Ine ndidzakulanditsa, ndipo udzandilemekeza.”
njalo lize kimi mhla lisekuhluphekeni; ngizalikhulula, lani lizangidumisa.”
16 Koma kwa woyipa, Mulungu akuti, “Kodi uli ndi mphamvu yanji kuti uzinena malamulo anga kapena kutenga pangano langa pa milomo yako?
Kodwa kwababi, uNkulunkulu uthi: “Lilelungelo bani ukukhuluma imithetho yami kumbe liphathe isivumelwano sami ezindebeni zenu na?
17 Iwe umadana ndi malangizo anga ndipo umaponyera kumbuyo kwako mawu anga.
Liyazizonda iziqondiso zami, lilahlela amazwi ami emuva kwenu.
18 Ukaona wakuba umamutsatira, umachita maere ako pamodzi ndi achigololo
Lithi lingabona isela lihle libambane lalo; lisuka lingenelane lezifebe.
19 Umagwiritsa ntchito pakamwa pako pa zinthu zoyipa ndipo umakonza lilime lako kuchita chinyengo.
Lisebenzisa imilomo yenu ukukhuluma okubi lifundise ulimi lwenu inkohliso.
20 Nthawi zonse umayankhula motsutsana ndi mʼbale wako ndipo umasinjirira mwana wa amayi ako enieni.
Linyeya umfowenu njalonjalo, limgcone umntakanyoko uqobo.
21 Wachita zimenezi ndipo Ine ndinali chete; umaganiza kuti ndine wofanana nawe koma ndidzakudzudzula ndipo ndidzakutsutsa pamaso pako.
Lizenzile lezizinto ngazithulela; lalikhumbula ukuthi ngifana lani. Kodwa ngizalikhuza ngilibonisa icala lenu obala.
22 “Ganizira izi, iwe amene umayiwala Mulungu kuti ndingakukadzule popanda wokupulumutsa:
Nanzelelani lokhu, lina elikhohlwa uNkulunkulu, funa ngilidabudabule, kungekho ongalilamulela:
23 Iye amene amapereka nsembe yamayamiko amandilemekeza, ndipo amakonza njira zake kuti ndimuonetse chipulumutso cha Mulungu.”
Lowo onikela iminikelo yokubonga uyangidumisa, njalo ulungisa indlela ukuze ngimtshengise insindiso yami.”

< Masalimo 50 >