< Masalimo 50 >

1 Salimo la Asafu. Wamphamvuyo, Yehova Mulungu, akuyankhula ndi kuyitanitsa dziko lapansi kuyambira kotulukira dzuwa mpaka kumene limalowera.
[Psalm lal Asaph] LEUM GOD, God Kulana, El kaskas; El pangon faclu nufon, mutawauk kutulap na nwe roto.
2 Kuchokera ku Ziyoni, mokongola kwambiri Mulungu akuwala.
Kalem lun God saromrom Zion me, Siti se su oaskulana in woiya.
3 Mulungu wathu akubwera ndipo sadzakhala chete; moto ukunyeketsa patsogolo pake, ndipo pomuzungulira pali mphepo yamkuntho
God lasr El tuku, tuh El tia tuku misla; Sie e lulap fah fahsr meet lukel, Ac sie eng upa raunella.
4 Iye akuyitanitsa zamumlengalenga ndi za pa dziko lapansi kuti aweruze anthu ake.
El pangon kusrao ac faclu elos in orek loh kac, Ac liye ke El ac nununku mwet lal.
5 Mundisonkhanitsire okhulupirika anga, amene anachita pangano ndi ine pochita nsembe.
El fahk ouinge, “Eisani mwet oaru luk nu yuruk, Elos su tuh orek wulela yuruk ke mwe kisa.”
6 Ndipo mayiko akumwamba akulengeza chilungamo chake, pakuti Mulungu mwini ndi woweruza.
Kusrao fahkak lah God El suwoswos, Ac El sifacna pa Mwet Nununku.
7 Imvani inu anthu anga, ndipo Ine ndidzayankhula, iwe Israeli, ndipo Ine ndidzayankhula mokutsutsa; ndine Mulungu, Mulungu wako.
“Porongo, kowos mwet luk, ac nga ac fah kaskas; Nga fah kaskas lain kom, Israel. Tuh nga God, God lom.
8 Sindikudzudzula chifukwa cha nsembe zako, kapena nsembe zako zopsereza zimene zili pamaso panga nthawi zonse.
Ke nga kai kom, tia ma ke sripen mwe kisa lom Ku ke mwe kisa firir su kom use nu sik pacl e nukewa.
9 Ine sindikufuna ngʼombe yayimuna kuchokera mʼkhola lako kapena mbuzi za mʼkhola lako,
Tusruktu nga tia enenu cow mukul liki ima lom, Ku nani liki un kosro nutum.
10 pakuti nyama iliyonse yakunkhalango ndi yanga ndiponso ngʼombe za ku mapiri ochuluka.
Kosro nukewa insak uh ma nutik, Ac oayapa cow su muta fin tausin inging.
11 Ine ndimadziwa mbalame iliyonse mʼmapiri ndiponso zolengedwa zonse zakutchire ndi zanga.
Won lemnak nukewa ma nutik Ac ma moul nukewa in imae.
12 Ndikanakhala ndi njala sindikanakuwuzani, pakuti dziko lonse ndi zonse zimene zili mʼmenemo ndi zanga.
“Nga fin masrinsral, nga ac tia siyuk sum ke mwe mongo, Mweyen faclu ac koano nufon ma luk.
13 Kodi ndimadya nyama ya ngʼombe zazimuna kapena kumwa magazi a mbuzi?
Ya nga kang ikwen cow mukul uh, Ku nim srahn nani uh?
14 “Pereka nsembe zachiyamiko kwa Mulungu, kwaniritsa malonjezo ako kwa Wammwambamwamba.
Nga God Fulatlana! Pa inge mwe kisa ma nga enenu sum: In sang kulo ke insiom, ac in akfalye ma kom wulela kac.
15 Ndipo undiyitane pa tsiku lako la masautso; Ine ndidzakulanditsa, ndipo udzandilemekeza.”
Pre nu sik ke pacl mwe ongoiya sikyak; Nga ac fah molikomla, Ac kom fah kaksakinyu.”
16 Koma kwa woyipa, Mulungu akuti, “Kodi uli ndi mphamvu yanji kuti uzinena malamulo anga kapena kutenga pangano langa pa milomo yako?
A God El fahk nu sin mwet koluk, “Efu ku kom in fahkak ma sap luk? Efu ku kom in sramsram ke wulela luk?
17 Iwe umadana ndi malangizo anga ndipo umaponyera kumbuyo kwako mawu anga.
Kom tia lungse nga in aksuwosye kom; Kom pilesru ma sap luk.
18 Ukaona wakuba umamutsatira, umachita maere ako pamodzi ndi achigololo
Kom asruoki nu sin mwet pisrapasr nukewa kom liye, Ac kom insese yurin mukul ac mutan su tia karinganang wulela in marut la.
19 Umagwiritsa ntchito pakamwa pako pa zinthu zoyipa ndipo umakonza lilime lako kuchita chinyengo.
“Pacl nukewa kom akola in kaskas koluk, Ac kom tia tupwek in kaskas kikiap.
20 Nthawi zonse umayankhula motsutsana ndi mʼbale wako ndipo umasinjirira mwana wa amayi ako enieni.
Kom akola in akkolukye mwet lom sifacna, Ac suk mwatan mwet lim.
21 Wachita zimenezi ndipo Ine ndinali chete; umaganiza kuti ndine wofanana nawe koma ndidzakudzudzula ndipo ndidzakutsutsa pamaso pako.
Kom oru ma inge nukewa, ac nga tia fahk kutena ma, Pwanang kom nunku mu nga oana kom. Tusruktu inge nga kai kom kac Tuh in kalem sum.
22 “Ganizira izi, iwe amene umayiwala Mulungu kuti ndingakukadzule popanda wokupulumutsa:
“Porongo ma inge, kowos su pilesreyu. Kowos fin tia, nga fah kunauskowosla, Na wangin sie ac fah molikowosla.
23 Iye amene amapereka nsembe yamayamiko amandilemekeza, ndipo amakonza njira zake kuti ndimuonetse chipulumutso cha Mulungu.”
Sang kulo pa mwe kisa se ma akfulatyeyu, Ac nga fah molelosla nukewa su akosyu.”

< Masalimo 50 >