< Masalimo 49 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la ana a Kora. Imvani izi anthu a mitundu yonse; mvetserani, nonse amene mumakhala pa dziko lonse,
Přednímu kantoru z synů Chóre, žalm. Slyšte to všickni národové, pozorujte všickni obyvatelé zemští.
2 anthu wamba pamodzi ndi anthu odziwika, olemera pamodzinso ndi osauka:
Tak z lidu obecného, jako z povýšených, tak bohatý, jako chudý.
3 Pakamwa panga padzayankhula mawu anzeru; mawu ochokera mu mtima mwanga adzapereka nzeru.
Ústa má mluviti budou moudrost, a přemyšlování srdce mého rozumnost.
4 Ndidzatchera khutu langa ku mwambo, ndi pangwe ndidzafotokoza momveka mwambi wanga.
Nakloním k přísloví ucha svého, a při harfě vykládati budu přípovídku svou.
5 Ine ndichitirenji mantha pamene masiku oyipa afika, pamene achinyengo oyipa andizungulira.
I proč se báti mám ve dnech zlých, aby nepravost těch, kteříž mi na paty šlapají, mne obklíčiti měla?
6 Iwo amene adalira kulemera kwawo ndi kutamandira kuchuluka kwa chuma chawo?
Kteříž doufají v svá zboží, a množstvím bohatství svého se chlubí.
7 Palibe munthu amene angawombole moyo wa mnzake kapena kuperekera mnzake dipo kwa Mulungu.
Žádný bratra svého nijakž vykoupiti nemůže, ani Bohu za něj dáti mzdy vyplacení,
8 Dipo la moyo ndi la mtengowapatali, palibe malipiro amene angakwanire,
(Neboť by velmi drahé musilo býti vyplacení duše jejich, protož nedovedeť toho na věky),
9 kuti iye akhale ndi moyo mpaka muyaya ndi kusapita ku manda.
Aby živ byl věčně, a neviděl porušení.
10 Pakuti onse amaona kuti anthu anzeru amamwalira; opusa ndi opanda nzeru chimodzimodzinso amawonongeka ndipo amasiyira chuma chawo anthu ena.
Nebo se vídá, že i moudří umírají, blázen a hovadný člověk zaroveň hynou, zboží svého i cizím zanechávajíce.
11 Manda awo adzakhala nyumba zawo mpaka muyaya, malo awo okhalako kwa nthawi yonse ya mibado yawo, ngakhale anatchula malo mayina awo.
Myšlení jejich jest, že domové jejich věční jsou, a příbytkové jejich od národu do pronárodu; pročež je po krajinách nazývají jmény svými.
12 Ngakhale munthu akhale wachuma chotani, adzafa ngati nyama.
Ale člověk v slávě netrvá, jsa podobný hovadům, kteráž hynou.
13 Izi ndi zimene zimachitikira iwo amene amadzidalira okha, ndi owatsatira awo amene amavomereza zimene amayankhula. (Sela)
Taková snažnost jejich jest bláznovstvím při nich, však potomci jejich ústy svými to schvalují. (Sélah)
14 Monga nkhosa iwo ayenera kupita ku manda, ndipo imfa idzawadya. Olungama adzawalamulira mmawa; matupi awo adzavunda mʼmanda, kutali ndi nyumba zawo zaufumu. (Sheol h7585)
Jako hovada v pekle skladeni budou, smrt je žráti bude, ale upřímí panovati budou nad nimi v jitře; způsob pak oněchno aby zvetšel, z příbytku svého octnou se v hrobě. (Sheol h7585)
15 Koma Mulungu adzawombola moyo wanga kuchoka ku manda; ndithu Iye adzanditengera kwa Iye mwini. (Sheol h7585)
Ale Bůh vykoupí duši mou z moci pekla, když mne přijme. (Sélah) (Sheol h7585)
16 Usavutike mu mtima pamene munthu akulemera, pamene ulemerero wa nyumba yake ukuchulukirachulukira;
Neboj se, když by někdo zbohatl, a když by se rozmnožila sláva domu jeho.
17 Pakuti sadzatenga kanthu pamodzi naye pamene wamwalira, ulemerero wake sudzapita pamodzi naye.
Při smrti zajisté ničeho nevezme, aniž sstoupí za ním sláva jeho.
18 Ngakhale pamene munthuyo ali moyo amadziyesa wodala, ndipo ngakhale atamandidwe pamene zinthu zikumuyendera bwino,
Ačťkoli duši své, pokudž jest živ, lahodí; k tomu chválí jej i jiní, když sobě čistě povoluje:
19 iyeyo adzakakhala pamodzi ndi mʼbado wa makolo ake, amene sadzaonanso kuwala.
A však musí se odebrati za věkem otců svých, a na věky světla neuzří.
20 Munthu amene ali ndi chuma koma wopanda nzeru adzafa ngati nyama yakuthengo.
Summou: Èlověk jsa ve cti, neusrozumí-li sobě, bývá učiněn podobný hovadům, kteráž hynou.

< Masalimo 49 >