< Masalimo 49 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la ana a Kora. Imvani izi anthu a mitundu yonse; mvetserani, nonse amene mumakhala pa dziko lonse,
Nangmih thlangkhqi boeih aw, ve ve za unawh taw; ve khawmdek awh ak awmkhqi boeih aw ngai lah uh,
2 anthu wamba pamodzi ndi anthu odziwika, olemera pamodzinso ndi osauka:
Ak nem ak sang, boei khawdengkhqi boeih:
3 Pakamwa panga padzayankhula mawu anzeru; mawu ochokera mu mtima mwanga adzapereka nzeru.
Kam kha ing cyihnaak awi kqawn kawmsaw; kak kawlung khuiawh kaw awi ing zaksimnaak ni pe kaw.
4 Ndidzatchera khutu langa ku mwambo, ndi pangwe ndidzafotokoza momveka mwambi wanga.
Awicyih benna kang haa keng kawng nyng saw; tingtoeng ing kak awi rylh ce kqawncaih kawng nyng.
5 Ine ndichitirenji mantha pamene masiku oyipa afika, pamene achinyengo oyipa andizungulira.
Khawnghi amak leek a pha law awh kawtih kqih nawh, qaai ak kqawn thlakche khqi –
6 Iwo amene adalira kulemera kwawo ndi kutamandira kuchuluka kwa chuma chawo?
a mimah a boeinaak ak ypnaak thlangkhqi ingkaw a boeinaak awh ak oek qu thlangkhqi ing anik chung khoep awh kawtih kak kqih kaw?
7 Palibe munthu amene angawombole moyo wa mnzake kapena kuperekera mnzake dipo kwa Mulungu.
U ingawm thlang a hqingnaak am hul thai nawh anih aham Khawsa venawh hulnaak a phu awm am pe thai hy-
8 Dipo la moyo ndi la mtengowapatali, palibe malipiro amene angakwanire,
hqing thaawngnaak a phu ve tlo soeih nawh, ikawmyih a phu pek ingawm am khoek nawh-
9 kuti iye akhale ndi moyo mpaka muyaya ndi kusapita ku manda.
thlang ing kumqui dy hqing nawh ama thu naak aham.
10 Pakuti onse amaona kuti anthu anzeru amamwalira; opusa ndi opanda nzeru chimodzimodzinso amawonongeka ndipo amasiyira chuma chawo anthu ena.
Thlakcyi a thih awm thlang boeih ing hu hy; thlak qaw ikaw amak sim thlang ing ang amyihna qeeng haih unawh thlang aham nani kawn ce ami ceh taak uh.
11 Manda awo adzakhala nyumba zawo mpaka muyaya, malo awo okhalako kwa nthawi yonse ya mibado yawo, ngakhale anatchula malo mayina awo.
A mimah ingtaw a mimah ang ming ing qamkhqi ce ta lawt hlai uhy, ami phyikhqi ni kumqui dy ami awmnaak imkhqi na awm nawh, amak dyt qoe ami cadil dyna ami awmnaak hun na awm loet hy.
12 Ngakhale munthu akhale wachuma chotani, adzafa ngati nyama.
Thlanghqing ve, boei seiawm, am cak loet hy; qamsa ak qeeng ing ni a ming myih hy.
13 Izi ndi zimene zimachitikira iwo amene amadzidalira okha, ndi owatsatira awo amene amavomereza zimene amayankhula. (Sela)
Amah ingkaw amah ak yp qunaak khqi taw cemyihna awm kawm uh, anih ak awi cangna nawh anih a hu awh ak bat thlangkhqi awm cemyihna awm kawm uh.
14 Monga nkhosa iwo ayenera kupita ku manda, ndipo imfa idzawadya. Olungama adzawalamulira mmawa; matupi awo adzavunda mʼmanda, kutali ndi nyumba zawo zaufumu. (Sheol h7585)
Tuu amyihna cekkhqi a dytnaak taw phyi mai ni, thihnaak ing a mingmih ce hqin khqi kaw. Thlak dyngkhqi ing cekkhqi ce mymcang hqit awh uk kawm usaw; cekkhqi a myi ce phyi awh ni a thu hly, a boeinaak im nu awhkawng hla hawh kaw. (Sheol h7585)
15 Koma Mulungu adzawombola moyo wanga kuchoka ku manda; ndithu Iye adzanditengera kwa Iye mwini. (Sheol h7585)
Cehlai, Khawsa ing ka hqingnaak ve phyi khui awhkawng thaawng kawmsaw; amah a venna ni ceh pyi kaw. (Sheol h7585)
16 Usavutike mu mtima pamene munthu akulemera, pamene ulemerero wa nyumba yake ukuchulukirachulukira;
Thlang ce khawhthem zen nawh, a ip khuiawh ik-oeih a taai law awh ce koeh kqih paqap;
17 Pakuti sadzatenga kanthu pamodzi naye pamene wamwalira, ulemerero wake sudzapita pamodzi naye.
A thih awhkaw pynoet ca awm khyn vang am ti a he hy, a taak khawhthem ing am nuk hqut tikaw.
18 Ngakhale pamene munthuyo ali moyo amadziyesa wodala, ndipo ngakhale atamandidwe pamene zinthu zikumuyendera bwino,
A hqing tloek awhtaw a zoseen soeih na ngai qu nawh – na boei tloek awhtaw thlang ing nim kyih hlai hy-
19 iyeyo adzakakhala pamodzi ndi mʼbado wa makolo ake, amene sadzaonanso kuwala.
a pakhqi a cadil ce ni ak bawng hly lawt hy, hqing vangnaak am hu voel qoe tikaw.
20 Munthu amene ali ndi chuma koma wopanda nzeru adzafa ngati nyama yakuthengo.
Zaaksimnaak taak kaana ak boei thlang taw qamsa ak qeeng ing ni a ning myih.

< Masalimo 49 >