< Masalimo 48 >
1 Nyimbo. Salimo la ana a Kora. Wamkulu ndi Yehova, ndi woyenera kwambiri matamando mu mzinda wa Mulungu wathu, phiri lake loyera.
Gamhanan si Jehova, ug dalayegon gayud sa pag-ayo, Sa ciudad sa atong Dios, sa iyang bukid nga balaan.
2 Lokongola mu utali mwake, chimwemwe cha dziko lonse lapansi. Malo aatali kwambiri a Zafoni ndiye Phiri la Ziyoni, mzinda wa Mfumu yayikulu.
Matahum sa gitas-on, ang kalipay sa tibook nga yuta. Mao ang bukid sa Sion, sa mga dapit sa amihanan. Ang ciudad sa gamhanang Hari.
3 Mulungu ali mu malinga ake; Iye wadzionetsa yekha kuti ndiye malinga akewo.
Ang Dios nagpaila sa iyang kaugalingon sa mga palacio niini nga maoy dalangpanan.
4 Pamene mafumu anasonkhana pamodzi, pamene anayendera pamodzi kudzalimbana nafe,
Kay, ania karon, ang mga hari manag-alirong sa ilang kaugalingon, (Sila) ming-agi sa tingub.
5 iwo anaona mzindawo ndipo anadabwa kwambiri; anathawa ndi mantha aakulu.
Nakakita (sila) niini, unya (sila) nanghibulong; Nangalisang (sila) nangalagiw (sila) sa pagdali.
6 Pomwepo anagwidwa nako kunjenjemera, ululu wonga wa mkazi woyembekezera pa nthawi yochira.
Ang panagkurog didto mingdakup kanila, Kasakit, ingon sa usa ka babaye nga nagaanak.
7 Inu munawawononga monga sitima zapamadzi za ku Tarisisi zitawonongeka ndi mphepo ya kummawa.
Uban sa hangin sa timogan. Ginaguba mo ang mga sakayan sa Tarsis.
8 Monga momwe tinamvera, kotero ife tinaona mu mzinda wa Yehova Wamphamvuzonse, mu mzinda wa Mulungu wathu. Mulungu adzawuteteza kwamuyaya.
Ingon sa among nadungog mao man ang among nakita Sa ciudad ni Jehova sa mga panon, sa ciudad sa atong Dios: Ang Dios magapahamutang niini sa walay katapusan. (Selah)
9 Mʼkati mwa Nyumba yanu Mulungu, ife timalingaliramo zachikondi chanu chosasinthika.
Nagapalandong kami sa imong mahigugmaong-kalolot, Oh Dios, Diha sa kinataliwad-an sa imong templo.
10 Monga dzina lanu, Inu Mulungu, matamando anu amafika ku malekezero a dziko lapansi dzanja lanu lamanja ladzaza ndi chilungamo.
Ingon sa imong ngalan; Oh Dios, Mao usab ang imong pagdayeg ngadto sa mga kinatumyan sa yuta: Ang imong toong kamot napuno sa pagkamatarung.
11 Phiri la Ziyoni likukondwera, midzi ya Yuda ndi yosangalala chifukwa cha maweruzo anu.
Palipaya ang bukid sa Sion, Pamayaa ang mga anak nga babaye sa Juda, Tungod sa imong mga paghukom.
12 Yendayendani mu Ziyoni, uzungulireni mzindawo, werengani nsanja zake.
Manlakaw kamo sa paglibut sa Sion, ug libuton ninyo siya; Isipa ninyo ang iyang mga torre;
13 Yangʼanitsitsani bwino mipanda yake, penyetsetsani malinga ake, kuti mudzafotokoze za izo ku mʼbado wotsatira.
Larawa pag-ayo ang iyang mga kuta; Sud-onga ang iyang mga palacio: Aron ikasugilon ninyo sa kaliwatan nga umalabut.
14 Pakuti Mulungu uyu ndi Mulungu wathu ku nthawi zosatha; Iye adzakhala mtsogoleri wathu mpaka ku mapeto.
Kay kining Dios mao ang atong Dios sa mga katuigan nga walay katapusan: Siya mao ang atong magmamando bisan hangtud sa kamatayon.