< Masalimo 47 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la ana a Kora. Ombani mʼmanja, inu anthu onse; fuwulani kwa Mulungu ndi mawu achimwemwe.
Aka mawt ham Korah ca rhoek kah Tingtoenglung Pilnam boeih loh kut paeng uh lamtah tamlung ol neh Pathen taengah yuhui uh lah.
2 Ndi woopsadi Yehova Wammwambamwamba; Mfumu yayikulu ya dziko lonse lapansi!
Khohni Yahweh tah rhih om tloe tih diklai pum kah manghai tanglue la om.
3 Iye anatigonjetsera mitundu yambirimbiri ya anthu; anayika anthu pansi pa mapazi athu.
Pilnam rhoek te mamih hmuila, namtu rhoek te mamih kho hmuila a hlak.
4 Iye anatisankhira cholowa chathu, chonyaditsa cha Yakobo, amene anamukonda. (Sela)
A lungnah Jakob kah a mingthennah, mamih kah rho te mamih ham a tuek. (Selah)
5 Mulungu wakwera, anthu akumufuwulira mwachimwemwe, Yehova wakwera, akumuyimbira malipenga.
Pathen tah tamlung neh, BOEIPA tah tuki ol neh luei coeng.
6 Imbani matamando kwa Mulungu, imbani matamando; imbani matamando kwa mfumu yathu, imbani matamando.
Pathen te tingtoeng uh, tingtoeng uh, mamih kah manghai te tingtoeng uh, tingtoeng uh.
7 Pakuti Mulungu ndi mfumu ya dziko lonse lapansi; imbirani Iye salimo la matamando.
Diklai pum kah Pathen Manghai he hlohlai neh tingtoeng uh.
8 Mulungu akulamulira mitundu ya anthu; Mulungu wakhala pa mpando wake waufumu woyera.
Pathen tah Namtom boeih soah manghai coeng tih Pathen tah amah kah hmuencim ngolkhoel dongah ngol.
9 Anthu otchuka mwa anthu a mitundu ina asonkhana monga anthu a Mulungu wa Abrahamu, pakuti mafumu a dziko lapansi ndi ake a Mulungu; Iye wakwezedwa kwakukulu.
Diklai photling rhoek he Pathen hut la om tih a thueng soeh dongah pilnam hlangcong rhoek loh Abraham Pathen kah pilnam a tingtun thiluh.

< Masalimo 47 >