< Masalimo 43 >
1 Onetsani kusalakwa kwanga Inu Mulungu; ndipo mundinenere mlandu wanga kutsutsana ndi mtundu wosapembedza; mundilanditse mʼmanja mwa achinyengo ndi anthu oyipa.
Wundungisa, a Nzambi, ayi wunzonzila mu mambu mama kuidi dikanda di batu dinkambu kinzikanga mambu maku. Wukhula mu batu ba luvunu ayi batu bambimbi.
2 Pajatu Inu Mulungu ndinu mphamvu zanga. Nʼchifukwa chiyani mwandikana ine? Nʼchifukwa chiyani ndiyenera kuyenda ndikulira, woponderezedwa ndi mdani?
Ngeyo Nzambi, ngeyo zingolo ziama. Bila mbi wundozidi e? Bila mbi mfueti diatilanga mu phasi, yamusungu kuidi mbeni e?
3 Tumizani kuwunika kwanu ndi choonadi chanu kuti zinditsogolere; mulole kuti zindifikitse ku phiri lanu loyera, kumalo kumene inu mumakhala.
Fidisa kiezila ayi Kiedika kiaku; bila bindiatisa, bika bindata ku mongo aku wunlongo ayi nate ku buangu kioki weti vuanda.
4 Ndipo ndidzapita ku guwa lansembe la Mulungu, kwa Mulungu, chimwemwe changa ndi chikondwerero changa. Ndidzakutamandani ndi zeze, Inu Mulungu wanga.
Buna ndiela kuenda ku ntala wu Nzambi; kuidi Nzambi khini ama ayi yangalala kuama. Buna ndiela kunzitisa mu ngitala, A Nzambi, Nzambi ama.
5 Nʼchifukwa chiyani uli ndi chisoni iwe moyo wanga? Nʼchifukwa chiyani wakhumudwa iwe mʼkati mwanga? Khulupirira Mulungu, pakuti ndidzamutamandabe Iye, Mpulumutsi wanga ndi Mulungu wanga.
Bila mbi vongidi bobo, a muelꞌala e? Bila mbi wulembo niongina mu khati ama e? Tula diana diaku mu Nzambi bila ndiela kunzitisa diaka, Mvulusi ama ayi Nzambi ama.