< Masalimo 43 >

1 Onetsani kusalakwa kwanga Inu Mulungu; ndipo mundinenere mlandu wanga kutsutsana ndi mtundu wosapembedza; mundilanditse mʼmanja mwa achinyengo ndi anthu oyipa.
Tuomitse minua, Jumala, ja ratkaise minun asiani armotointa kansaa vastaan, ja päästä minua kavaloista ja vääristä ihmisistä.
2 Pajatu Inu Mulungu ndinu mphamvu zanga. Nʼchifukwa chiyani mwandikana ine? Nʼchifukwa chiyani ndiyenera kuyenda ndikulira, woponderezedwa ndi mdani?
Sillä sinä olet minun väkevyyteni Jumala, miksis syökset minun pois? miksis minun annat murheissani käydä, koska vihollinen minua ahdistaa?
3 Tumizani kuwunika kwanu ndi choonadi chanu kuti zinditsogolere; mulole kuti zindifikitse ku phiri lanu loyera, kumalo kumene inu mumakhala.
Lähetä valkeutes ja totuutes minua saattamaan, ja tuomaan sinun pyhän vuores tykö ja sinun asumises tykö.
4 Ndipo ndidzapita ku guwa lansembe la Mulungu, kwa Mulungu, chimwemwe changa ndi chikondwerero changa. Ndidzakutamandani ndi zeze, Inu Mulungu wanga.
Ja minä kävisin sisälle Jumalan alttarin tykö, sen Jumalan tykö, joka minun iloni ja riemuni on, ja kiittäisin sinua kanteleilla, Jumalani, minun Jumalani.
5 Nʼchifukwa chiyani uli ndi chisoni iwe moyo wanga? Nʼchifukwa chiyani wakhumudwa iwe mʼkati mwanga? Khulupirira Mulungu, pakuti ndidzamutamandabe Iye, Mpulumutsi wanga ndi Mulungu wanga.
Mitäs murehdit, sieluni, ja olet minussa niin levotoin? Turvaa Jumalaan; sillä minä vielä nytkin häntä kiitän, että hän on minun kasvoini apu ja minun Jumalani.

< Masalimo 43 >