< Masalimo 43 >

1 Onetsani kusalakwa kwanga Inu Mulungu; ndipo mundinenere mlandu wanga kutsutsana ndi mtundu wosapembedza; mundilanditse mʼmanja mwa achinyengo ndi anthu oyipa.
O Elohim Pathen themmona bei kahi neiphongdoh in! Elohim Pathen ginglou hoa kon in nei vengdoh in, chutengleh mikitah lou holeh joupan hoa kon in neihuhdoh in.
2 Pajatu Inu Mulungu ndinu mphamvu zanga. Nʼchifukwa chiyani mwandikana ine? Nʼchifukwa chiyani ndiyenera kuyenda ndikulira, woponderezedwa ndi mdani?
Ajeh chu nanghi kakiselna Pathen Elohim nahi, ibol a neipaidoh hitam? Ibol a keima kadougal ten eibolset jeh a lunggim a kava lele dingham?
3 Tumizani kuwunika kwanu ndi choonadi chanu kuti zinditsogolere; mulole kuti zindifikitse ku phiri lanu loyera, kumalo kumene inu mumakhala.
Nadih na le navah na chu neihinsol peh in, hichun eilamhil hen. Hihochun nangma chenna muol theng chu eilhut hen.
4 Ndipo ndidzapita ku guwa lansembe la Mulungu, kwa Mulungu, chimwemwe changa ndi chikondwerero changa. Ndidzakutamandani ndi zeze, Inu Mulungu wanga.
Hikomma chun keima Elohim Pathen maicham achu kasemjang puma kathang vahding ahi, O Pathen Elohim.
5 Nʼchifukwa chiyani uli ndi chisoni iwe moyo wanga? Nʼchifukwa chiyani wakhumudwa iwe mʼkati mwanga? Khulupirira Mulungu, pakuti ndidzamutamandabe Iye, Mpulumutsi wanga ndi Mulungu wanga.
Idia lungkham kahim? Ipidinga kalung lhadah ham? Keiman kakinepna Elohim Pathen a koi inge! Eihuhhingpa le Elohim ka Pathen keiman nangma thangvah kit inge!

< Masalimo 43 >