< Masalimo 4 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe wa zida za zingwe. Salimo la Davide. Ndiyankheni pamene ndiyitana Inu, Inu Mulungu wa chilungamo changa. Pumulitseni ku zowawa zanga; chitireni chifundo ndi kumva pemphero langa.
KOT kapung pa i, kom kotin mangi ia ni ai likelikwir. Pwe kom kin kotin kamait ia la ni ai ansau apwal. Kom kotin maki ong ia o mangi ai kapakap.
2 Anthu inu, mpaka liti mudzakhala mukusandutsa ulemerero wanga kukhala manyazi? Mpaka liti mudzakonda zachabe ndi kufuna milungu yabodza? (Sela)
Komail saumas akan! Arai da mar ai pan susued? Arai da omail pok ong me mal kot, o omail perenki likam? (Sela)
3 Dziwani kuti Yehova wadziyikira padera anthu okhulupirika; Yehova adzamva pamene ndidzamuyitana.
Komail lolekongala, ap asa, me Ieowa kotin piladar sapwilim a lelapok o. Ieowa kin kotin mangi ia ni ai likelikwir ong i.
4 Kwiyani koma musachimwe; pamene muli pa mabedi anu, santhulani mitima yanu ndi kukhala chete. (Sela)
Ni omail makar, komail der wia dip. Komail madamadauaki mongiong omail ni omail wendi pon los o ap auiaui. (Sela)
5 Perekani nsembe zolungama ndipo dalirani Yehova.
Komail mairongki mairong pung o liki Ieowa.
6 Ambiri akufunsa kuti, “Ndani angationetse chabwino chilichonse?” Kuwunika kwa nkhope yanu kutiwalire, Inu Yehova.
Me toto kin inda: Is me pan kasale ong kitail me mau kan? A Ieowa, kom kotin kamaraine kin kit marain en silang omui!
7 Inu mwadzaza mtima wanga ndi chimwemwe chachikulu kuposa kuchuluka kwa tirigu wawo ndi vinyo watsopano.
Komui kotin kaperenda mongiong i laud sang ansaun arail wain o korn me toto.
8 Ine ndidzagona ndi kupeza tulo mwamtendere, pakuti Inu nokha, Inu Yehova, mumandisamalira bwino.
I kin wonon o mamair ni popol; pwe komui ta Maing, me kotin sauasa ia da, pwe i en kak moleilei.

< Masalimo 4 >