< Masalimo 4 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe wa zida za zingwe. Salimo la Davide. Ndiyankheni pamene ndiyitana Inu, Inu Mulungu wa chilungamo changa. Pumulitseni ku zowawa zanga; chitireni chifundo ndi kumva pemphero langa.
Til Sangmesteren; med Strengeleg; en Psalme af David.
2 Anthu inu, mpaka liti mudzakhala mukusandutsa ulemerero wanga kukhala manyazi? Mpaka liti mudzakonda zachabe ndi kufuna milungu yabodza? (Sela)
Naar jeg raaber, da bønhør mig, min Retfærdigheds Gud! i Trængsel skaffede du mig Rum; vær mig naadig og hør min Bøn!
3 Dziwani kuti Yehova wadziyikira padera anthu okhulupirika; Yehova adzamva pamene ndidzamuyitana.
I Menneskens Børn! hvor længe skal min Ære være til Skændsel? I elske Forfængelighed og søge Løgn. (Sela)
4 Kwiyani koma musachimwe; pamene muli pa mabedi anu, santhulani mitima yanu ndi kukhala chete. (Sela)
Vider dog, at Herren har udkaaret sin hellige; Herren hører, naar jeg raaber til ham.
5 Perekani nsembe zolungama ndipo dalirani Yehova.
Bliver vrede, men synder ikke; taler i eders Hjerte paa eders Leje; og værer stille! (Sela)
6 Ambiri akufunsa kuti, “Ndani angationetse chabwino chilichonse?” Kuwunika kwa nkhope yanu kutiwalire, Inu Yehova.
Ofrer Retfærdigheds Ofre, og forlader eder paa Herren!
7 Inu mwadzaza mtima wanga ndi chimwemwe chachikulu kuposa kuchuluka kwa tirigu wawo ndi vinyo watsopano.
Mange sige: Hvo vil vise os godt? Herre! opløft dit Ansigts Lys over os.
8 Ine ndidzagona ndi kupeza tulo mwamtendere, pakuti Inu nokha, Inu Yehova, mumandisamalira bwino.
Du gav Glæde i mit Hjerte større end den, de havde, da deres Korn og deres Most var i Overflod. I Fred vil jeg baade lægge mig og sove; thi du, Herre! skal lade mig bo ene i Tryghed.

< Masalimo 4 >