< Masalimo 38 >
1 Salimo la Davide. Kupempha. Yehova musandidzudzule mutapsa mtima kapena kundilanga muli ndi ukali.
Zabbuli ya Dawudi, ey’okujjukiza. Ayi Mukama tonnenya ng’okyaliko obusungu, oba okunkangavvula ng’oliko ekiruyi.
2 Pakuti mivi yanu yandilasa, ndipo dzanja lanu latsika ndipo landifikira.
Kubanga obusaale bwo bunfumise, n’omuggo gwo gunkubye nnyo.
3 Chifukwa cha ukali wanu mulibe thanzi mʼthupi langa; mafupa anga alibe mphamvu chifukwa cha tchimo langa.
Obusungu bwo bundwazizza nzenna, n’amagumba gange gonna gansagala olw’ebyonoono byange.
4 Kulakwa kwanga kwandipsinja ngati katundu wolemera kwambiri kuposa mphamvu zanga.
Omusango gwe nzizizza guyitiridde, gunzitoowerera ng’omugugu omunene oguteetikkika.
5 Mabala anga akuwola ndipo akununkha chifukwa cha uchitsiru wa moyo wanga wauchimo.
Ebiwundu byange bitanye era biwunya, olw’okwonoona kwange okw’obusirusiru.
6 Ine ndapindika msana ndipo ndawerama kwambiri; tsiku lonse ndimangolira.
Nkootakoota era mpweddemu ensa, ŋŋenda nsinda obudde okuziba.
7 Msana wanga wagwidwa ndi ululu wosasimbika, mulibe thanzi mʼthupi langa.
Omugongo gunnuma nnyo, ne mu mubiri gwange temukyali bulamu.
8 Ndilibe mphamvu ndipo ndakunthidwa kwathunthu; ndikubuwula ndi ululu wa mumtima.
Sikyalimu maanyi era nzenna mmenyesemenyese; nsinda buli bbanga olw’obulumi mu mutima.
9 Zokhumba zanga zonse zili poonekera pamaso panu Ambuye, kusisima kwanga sikunabisike kwa Inu.
Mukama, bye neetaaga byonna obimanyi, n’okusinda kwange okuwulira.
10 Mtima wanga ukugunda, mphamvu zanga zikutha; ngakhale kuwala kwachoka mʼmaso mwanga.
Omutima gumpejjawejja, amaanyi gampweddemu; n’okulaba sikyalaba.
11 Abwenzi anga ndi anzanga akundipewa chifukwa cha mabala anga; anansi anga akhala kutali nane.
Mikwano gyange ne be nayitanga nabo banneewala olw’amabwa gange; ne bannange tebakyansemberera.
12 Iwo amene akufunafuna moyo wanga atchera misampha yawo, oti andipwetekewo amayankhula za kuwonongeka kwanga; tsiku lonse amakonza zachinyengo.
Abaagala okunzita bantega emitego, n’abo abangigganya bateesa okummalawo. Buli bbanga baba bateesa kunkola kabi.
13 Ine ndili ngati munthu wosamva amene sangamve, monga wosayankhula, amene sangathe kutsekula pakamwa pake;
Ndi ng’omuggavu w’amatu, atawulira; nga kiggala, atayogera.
14 Ndakhala ngati munthu amene samva, amene pakamwa pake sipangathe kuyankha.
Nfuuse ng’omuntu atalina ky’awulira, atasobola kwanukula.
15 Ndikudikira Inu Yehova; mudzayankha, Inu Ambuye Mulungu wanga.
Ddala ddala nnindirira ggwe, Ayi Mukama, onnyanukule, Ayi Mukama Katonda wange.
16 Pakuti Ine ndinati, “Musawalole kuti akondwere kapena kudzikweza okha pa ine pamene phazi langa laterereka.”
Tobakkiriza kunneeyagalirako, oba okunneegulumirizaako ng’ekigere kyange kiseeredde.
17 Pakuti ndili pafupi kugwa, ndipo ndikumva kuwawa nthawi zonse.
Kubanga nsemberedde okugwa, era nga nnumwa buli kiseera.
18 Ndikuvomereza mphulupulu zanga; ndipo ndavutika ndi tchimo langa.
Ddala ddala njatula ebyonoono byange; nnumirizibwa ekibi kyange.
19 Ambiri ndi adani anga amphamvu; amene amandida popanda chifukwa alipo ochuluka kwambiri.
Abalabe bange bangi era ba maanyi; n’abo abankyayira obwereere bangi nnyo.
20 Iwo amene amandibwezera zoyipa mʼmalo mwa zabwino amandinyoza pamene nditsatira zabwino.
Abalabe bange bankyawa olw’okuba omulongoofu, era bwe nkola ebirungi banjogerako ebitasaana.
21 Inu Yehova, musanditaye; musakhale kutali ndi ine Mulungu wanga.
Ayi Mukama, tonjabulira; tobeera wala nange, Ayi Katonda wange.
22 Bwerani msanga kudzandithandiza, Inu Ambuye Mpulumutsi wanga.
Ayi Mukama Omulokozi wange, yanguwa okumbeera.