< Masalimo 38 >

1 Salimo la Davide. Kupempha. Yehova musandidzudzule mutapsa mtima kapena kundilanga muli ndi ukali.
Hina Gode! Dia ougiba: le, nama se bidi mae ima!
2 Pakuti mivi yanu yandilasa, ndipo dzanja lanu latsika ndipo landifikira.
Di da na Dia dadi amoga fa: ginisi, amola na fane sanasi.
3 Chifukwa cha ukali wanu mulibe thanzi mʼthupi langa; mafupa anga alibe mphamvu chifukwa cha tchimo langa.
Dia da nama ougiba: le, na se baligili nabala. Na wadela: i hou hamobeba: le, na da: i huluane da olo bagade madelasa.
4 Kulakwa kwanga kwandipsinja ngati katundu wolemera kwambiri kuposa mphamvu zanga.
Na da nina: wadela: i hamonana fedege agoane hano heda: i amoga gela daha. Na wadela: i hou da fedege agoane, liligi bagadedafa aguni masunu hamedei agoai ba: sa.
5 Mabala anga akuwola ndipo akununkha chifukwa cha uchitsiru wa moyo wanga wauchimo.
Bai na da gagaoule hamobeba: le, na aiya da dasale gahasa.
6 Ine ndapindika msana ndipo ndawerama kwambiri; tsiku lonse ndimangolira.
Na da se nabawane beguduli, gala: la sa: i. Na da hahabe asili daeya, mae fisili, dinana.
7 Msana wanga wagwidwa ndi ululu wosasimbika, mulibe thanzi mʼthupi langa.
Na da asugiba: le, da: i goaeasa. Amola na da bogomu gadenei ba: sa.
8 Ndilibe mphamvu ndipo ndakunthidwa kwathunthu; ndikubuwula ndi ululu wa mumtima.
Na da gasa hamedene, dafawane gala: la sa: i. Na da da: i dioi, amola se nababeba: le gayasa.
9 Zokhumba zanga zonse zili poonekera pamaso panu Ambuye, kusisima kwanga sikunabisike kwa Inu.
Hina Gode! Na hanai amo Dia dawa: ! Na gayabe huluane Dia naba!
10 Mtima wanga ukugunda, mphamvu zanga zikutha; ngakhale kuwala kwachoka mʼmaso mwanga.
Na habe da ha: ha: sa, amola na gasa da asi dagoi. Na si da mobi sa: i dagoi.
11 Abwenzi anga ndi anzanga akundipewa chifukwa cha mabala anga; anansi anga akhala kutali nane.
Na da aiya bagohame madelaiba: le, na sama amola na na: iyado fi dunu ilia da nama hame gadenena maha. Na sosogodafa amolalia na hagasa.
12 Iwo amene akufunafuna moyo wanga atchera misampha yawo, oti andipwetekewo amayankhula za kuwonongeka kwanga; tsiku lonse amakonza zachinyengo.
Dunu da na medole legemusa: dawa: be, ilia da na sa: ima: ne sanenisa. Amola dunu da nama se ima: ne dawa: be, ilia da na wadela: lesimusa: magagisa. Ilia da na wadela: lesimusa: sia: fane ilegesu hou hame yolesisa.
13 Ine ndili ngati munthu wosamva amene sangamve, monga wosayankhula, amene sangathe kutsekula pakamwa pake;
Na da ge ga: i dunu defele, hame naba. Amola na da sia: hamedei dunu agoane, hame sia: da.
14 Ndakhala ngati munthu amene samva, amene pakamwa pake sipangathe kuyankha.
Na da ge ga: iba: le, dabe adole imunu hamedei dunu agoai gala.
15 Ndikudikira Inu Yehova; mudzayankha, Inu Ambuye Mulungu wanga.
Hina Gode, na da dima dafawaneyale dawa: sa, amola Di da na Hina Godeba: le, nama dabe adole imunu.
16 Pakuti Ine ndinati, “Musawalole kuti akondwere kapena kudzikweza okha pa ine pamene phazi langa laterereka.”
Na da se nabasu baligilidafa nababeba: le, nama ha lai dunu da na mae habosesema: ma. Ilia da na dafai hou ba: beba: le, Dia mae habosesele sia: ma: ma!
17 Pakuti ndili pafupi kugwa, ndipo ndikumva kuwawa nthawi zonse.
Na da maedafa fisili, se naba. Amola na da dafamu gadenei ba: sa.
18 Ndikuvomereza mphulupulu zanga; ndipo ndavutika ndi tchimo langa.
Na da na wadela: i hou sisane fofada: sa. Be na da amo dawa: beba: le, bagadewane beda: sa.
19 Ambiri ndi adani anga amphamvu; amene amandida popanda chifukwa alipo ochuluka kwambiri.
Na ha lai dunu da dagumui noga: i amola gasa fi gala. Nama ha lai dunu bagohame da nama bai hamedene, higale ba: sa.
20 Iwo amene amandibwezera zoyipa mʼmalo mwa zabwino amandinyoza pamene nditsatira zabwino.
Dunu amo da noga: le hamobe dunuma wadela: i dabe iaha, ilia da na higale ba: sa. Bai na da moloi hou amoga hamomusa: , logo hogobeba: le.
21 Inu Yehova, musanditaye; musakhale kutali ndi ine Mulungu wanga.
Hina Gode! Dia na mae fisiagama! Na Gode! Nama gasigale mae aligima!
22 Bwerani msanga kudzandithandiza, Inu Ambuye Mpulumutsi wanga.
Hina Gode! Na Gaga: sudafa! Wahadafa, na fidima!

< Masalimo 38 >