< Masalimo 36 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide, mtumiki wa Yehova. Uthenga uli mu mtima mwanga wonena za kuchimwa kwa munthu woyipa: Mu mtima mwake mulibe kuopa Mulungu.
Aka mawt ham BOEIPA sal David kah Halang kah boekoek te ka thinko lungbuei khui kah olphong ah tah, a mik hmuh ah Pathen birhihnah khueh pawh.
2 Pakuti iye mʼkuona kwake amadzinyenga yekha kwambiri, sazindikira kapena kudana ndi tchimo lake.
A mik neh amah kathaesainah hmuh ham, ka thiinah tila amah te hoem.
3 Mawu a pakamwa pake ndi oyipa ndi achinyengo; iyeyo waleka kukhala wanzeru ndi kuchita zabwino.
A ka dongkah ol tah boethae neh thailatnah la coeng tih, a then te cangbam hamla a toeng.
4 Ngakhale ali pa bedi pake amakonzekera zoyipa; iye amadzipereka yekha ku njira ya uchimo ndipo sakana cholakwa chilichonse.
A thingkong dongah boethae te a moeh. Long then pawt ah pai tih a thae te hnawt pawh.
5 Chikondi chanu Yehova, chimafika ku mayiko a kumwamba, kukhulupirika kwanu mpaka ku mitambo.
Aw BOEIPA na sitlohnah loh vaan duela a pha. Na uepomnah loh khomong a pha.
6 Chilungamo chanu Mulungu chili ngati mapiri aakulu, chiweruzo chanu chili ngati kuzama kwakukulu. Yehova mumasunga munthu pamodzi ndi chinyama.
Na duengnah tah Pathen tlang bangla om tih na laitloeknah te dung tangkik. Hlang neh rhamsa he BOEIPA nang loh na khang.
7 Chikondi chanu chosatha ndi chamtengowapatali! Otchuka pamodzi ndi anthu wamba pakati pa anthu amapeza pothawirapo mu mthunzi wa mapiko anu.
Pathen namah kah sitlohnah he bahoeng a phu om tih hlang capa rhoek loh na phae hlip ah ying uh.
8 Iwo amadyerera zinthu zambiri za mʼnyumba yanu; Inu mumawapatsa chakumwa kuchokera mu mtsinje wanu wachikondwerero.
Na im kah maehhloi dongah hmilhmal uh tih namah kah omthennah soklong tui te amih na tul.
9 Pakuti kwa Inu kuli kasupe wamoyo; mʼkuwala kwanu ifenso timaona kuwala.
Namah taengah hingnah thunsih om tih, namah kah vangnah dongah vangnah ka hmuh uh.
10 Pitirizani chikondi chanu pa iwo amene amakudziwani, chilungamo chanu kwa olungama mtima.
Nang aka ming rhoek taengah na sitlohnah hing sak lamtah lungbuei aka thuem taengah na duengnah om sak.
11 Musalole kuti phazi la wodzikuza libwere kulimbana nane, kapena dzanja la oyipa kundithamangitsa.
Hoemnah kho loh kai m'pha boel saeh lamtah halang kut te kai taengah vikvawk boel saeh.
12 Onani momwe ochita zoyipa agonera atagwa, aponyeni pansi, kuti asathe kudzukanso!
Boethae aka saii rhoek te pahoi cungku uh tih a bung uh dongah tlai uh thai pawt lah ko.

< Masalimo 36 >