< Masalimo 34 >

1 Salimo la Davide. Pamene iye ananyengezera misala pamaso pa Abimeleki, amene anamupirikitsa, iyeyo nʼkuchoka. Ndidzayamika Yehova nthawi zonse; matamando ake adzakhala pa milomo yanga nthawi zonse.
to/for David in/on/with to change he [obj] taste his to/for face: before Abimelech and to drive out: drive out him and to go: went to bless [obj] LORD in/on/with all time continually praise his in/on/with lip my
2 Moyo wanga udzanyadira Yehova; anthu osautsidwa amve ndi kukondwera.
in/on/with LORD to boast: boast soul my to hear: hear poor and to rejoice
3 Lemekezani Yehova pamodzi ndi ine; tiyeni pamodzi tikuze dzina lake.
to magnify to/for LORD with me and to exalt name his together
4 Ine ndinafunafuna Yehova ndipo Iye anandiyankha; anandilanditsa ku mantha anga onse.
to seek [obj] LORD and to answer me and from all fear my to rescue me
5 Iwo amene amayangʼana kwa Iye, nkhope zawo zimanyezimira; nkhope zawo sizikhala zophimbidwa ndi manyazi.
to look to(wards) him and to shine and face their not be ashamed
6 Munthu wosauka uno anayitana, ndipo Yehova anamumva; Yehova anamupulumutsa ku mavuto ake onse.
this afflicted to call: call out and LORD to hear: hear and from all distress his to save him
7 Mngelo wa Yehova amatchinjiriza amene amakonda Iye ndi kuwalanditsa.
to camp messenger: angel LORD around to/for afraid his and to rescue them
8 Lawani ndipo onani kuti Yehova ndi wabwino; wodala munthu amene amathawira kwa Iye.
to perceive and to see: see for be pleasing LORD blessed [the] great man to seek refuge in/on/with him
9 Wopani Yehova inu oyera mtima ake, pakuti iwo amene amaopa Iye sasowa kanthu.
to fear: revere [obj] LORD holy: saint his for nothing need to/for afraid his
10 Mikango itha kulefuka ndi kumva njala koma iwo amene amafunafuna Yehova sasowa kanthu kalikonse kabwino.
lion be poor and be hungry and to seek LORD not to lack all good
11 Bwerani ana anga, mundimvere; ndidzakuphunzitsani kuopa Yehova.
to go: come! son: child to hear: hear to/for me fear LORD to learn: teach you
12 Aliyense wa inu amene amakonda moyo wake ndi kukhumba kuti aone masiku abwino ambiri,
who? [the] man [the] delighting life to love: lover day to/for to see: see good
13 asunge lilime lake ku zoyipa ndi milomo yake kuti isayankhule zonama.
to watch tongue your from bad: evil and lips your from to speak: speak deceit
14 Tembenuka kuchoka ku zoyipa ndipo chita zabwino; funafuna mtendere ndi kuwulondola.
to turn aside: remove from bad: evil and to make: do good to seek peace and to pursue him
15 Maso a Yehova ali pa olungama ndipo makutu ake ali tcheru kumva kulira kwawo;
eye LORD to(wards) righteous and ear his to(wards) cry their
16 nkhope ya Yehova ikutsutsana ndi amene amachita zoyipa, kuwachotsa kuti asawakumbukirenso pa dziko lapansi.
face LORD in/on/with to make: do bad: evil to/for to cut: eliminate from land: country/planet memorial their
17 Olungama amafuwula, ndipo Yehova amawamva; Iye amawalanditsa ku mavuto awo onse.
to cry and LORD to hear: hear and from all distress their to rescue them
18 Yehova ali pafupi kwa osweka mtima ndipo amapulumutsa iwo amene asweka mu mzimu.
near LORD to/for to break heart and [obj] contrite spirit to save
19 Munthu wolungama atha kukhala ndi mavuto ambiri, Koma Yehova amamulanditsa ku mavuto onsewo,
many distress: harm righteous and from all their to rescue him LORD
20 Iye amateteza mafupa ake onse, palibe limodzi la mafupawo limene lidzathyoledwa.
to keep: guard all bone his one from them not to break
21 Choyipa chidzapha anthu oyipa; adani a olungama adzapezeka olakwa.
to die wicked distress: harm and to hate righteous be guilty
22 Yehova amawombola atumiki ake; aliyense amene amathawira kwa Iye sadzapezeka wolakwa.
to ransom LORD soul: life servant/slave his and not be guilty all [the] to seek refuge in/on/with him

< Masalimo 34 >