< Masalimo 32 >

1 Salimo la Davide. Malangizo. Ngodala munthu amene zolakwa zake zakhululukidwa; amene machimo ake aphimbidwa.
Davut'un mezmuru - Maskil Ne mutlu isyanı bağışlanan, Günahı örtülen insana!
2 Ngodala munthu amene machimo ake Yehova sawawerengeranso pa iye ndipo mu mzimu mwake mulibe chinyengo.
Suçu RAB tarafından sayılmayan, Ruhunda hile bulunmayan insana ne mutlu!
3 Pamene ndinali chete, mafupa anga anakalamba chifukwa cha kubuwula kwanga tsiku lonse.
Sustuğum sürece Kemiklerim eridi, Gün boyu inlemekten.
4 Pakuti usana ndi usiku dzanja lanu linandipsinja; mphamvu zanga zinatha monga nthawi yotentha yachilimwe. (Sela)
Çünkü gece gündüz Elin üzerimde ağırlaştı. Dermanım tükendi yaz sıcağında gibi. (Sela)
5 Kotero ine ndinavomereza tchimo langa kwa Inu, sindinabise mphulupulu zanga. Ndinati, “Ine ndidzawulula zolakwa zanga kwa Yehova, ndipo Inu munandikhululukira mlandu wa machimo anga.” (Sela)
Günahımı açıkladım sana, Suçumu gizlemedim. “RAB'be isyanımı itiraf edeceğim” deyince, Günahımı, suçumu bağışladın. (Sela)
6 Choncho aliyense okhulupirika apemphere kwa Inuyo pomwe mukupezeka; ndithu pamene madzi amphamvu auka, sadzamupeza.
Bu nedenle her sadık kulun Ulaşılır olduğun zaman sana dua etsin. Engin sular taşsa bile ona erişemez.
7 Inu ndi malo anga obisala; muzinditeteza ku mavuto ndipo muzindizinga ndi nyimbo zachipulumutso. (Sela)
Sığınağım sensin, Beni sıkıntıdan korur, Çevremi kurtuluş ilahileriyle kuşatırsın. (Sela)
8 Ndidzakulangiza ndi kukuphunzitsa njira imene udzayendamo; ndidzakupatsa uphungu ndi kukuyangʼanira.
Eğiteceğim seni, gideceğin yolu göstereceğim, Öğüt vereceğim sana, Gözüm sendedir.
9 Usakhale ngati kavalo kapena bulu, zimene zilibe nzeru, koma ziyenera kuwongoleredwa ndi zitsulo za mʼkamwa ndi pamutu, ukapanda kutero sizibwera kwa iwe.
At ya da katır gibi anlayışsız olmayın; Onları idare etmek için gem ve dizgin gerekir, Yoksa sana yaklaşmazlar.
10 Zowawa ndi zambiri za anthu oyipa koma chikondi chosatha cha Yehova chimamuzinga munthu amene amadalira Iye.
Kötülerin acısı çoktur, Ama RAB'be güvenenleri O'nun sevgisi kuşatır.
11 Kondwerani mwa Yehova inu olungama; imbani, inu nonse amene muli owongoka mtima!
Ey doğru insanlar, sevinç kaynağınız RAB olsun, coşun; Ey yüreği temiz olanlar, Hepiniz sevinç çığlıkları atın!

< Masalimo 32 >