< Masalimo 32 >

1 Salimo la Davide. Malangizo. Ngodala munthu amene zolakwa zake zakhululukidwa; amene machimo ake aphimbidwa.
POMAIKAI ka mea i kalaia kona hala, I uhiia hoi koua hewa.
2 Ngodala munthu amene machimo ake Yehova sawawerengeranso pa iye ndipo mu mzimu mwake mulibe chinyengo.
Pomaikai ke kanaka, maluna ona ka hoili ole ia o ka hewa e Iehova. Iloko hoi o kona uhane aohe hookamani.
3 Pamene ndinali chete, mafupa anga anakalamba chifukwa cha kubuwula kwanga tsiku lonse.
I ko'u mumule ana ua elemakule ae la kuu mau iwi, I kuu auwe ana a po ka la.
4 Pakuti usana ndi usiku dzanja lanu linandipsinja; mphamvu zanga zinatha monga nthawi yotentha yachilimwe. (Sela)
No ka mea, i ke ao a me ka po, kaumaha mai la kou lima maluna iho o'u: Ua hooliloia ko'u ma-u ana i maloo o ka makalii. (Sila)
5 Kotero ine ndinavomereza tchimo langa kwa Inu, sindinabise mphulupulu zanga. Ndinati, “Ine ndidzawulula zolakwa zanga kwa Yehova, ndipo Inu munandikhululukira mlandu wa machimo anga.” (Sela)
Ua hai aku au i ko'u hewa ia oe; Aole au i huna i ko'u lawehala ana. I iho la an, E hai aku au i ko'u hala ia Iehova; A ua kala mai oe i ka hewa o ka'u lawehala ana. (Sila)
6 Choncho aliyense okhulupirika apemphere kwa Inuyo pomwe mukupezeka; ndithu pamene madzi amphamvu auka, sadzamupeza.
No ia mea, e pule aku ia oe na haipule i ka wa e loaa ai oe; Oiaio, i ke kahe aua o na wai nui, aole ia e kokoke ia ia.
7 Inu ndi malo anga obisala; muzinditeteza ku mavuto ndipo muzindizinga ndi nyimbo zachipulumutso. (Sela)
O oe no kuu wahi e pee ai; E hoopakele no oe ia'u i ka popilikia: E hoopuni no oe ia'u me na mele no ke ola. (Sila)
8 Ndidzakulangiza ndi kukuphunzitsa njira imene udzayendamo; ndidzakupatsa uphungu ndi kukuyangʼanira.
E ao aku au ia oe, a hoike ia oe i kou ala e hele ai; E alakai au ia oe me ko'u maka.
9 Usakhale ngati kavalo kapena bulu, zimene zilibe nzeru, koma ziyenera kuwongoleredwa ndi zitsulo za mʼkamwa ndi pamutu, ukapanda kutero sizibwera kwa iwe.
Mai hoohalike oukou me ka lio a me ka hoki, na mea ike ole; E pono ke kaohiia kona waha me ka haowaha, a me ke kaula waha, o hele kokoke ia ia oe.
10 Zowawa ndi zambiri za anthu oyipa koma chikondi chosatha cha Yehova chimamuzinga munthu amene amadalira Iye.
E nui auanei ka ehaeha o ka mea hewa; Aka, o ka mea hilinai ia Iehova. e hoopuniia no ia me ke aloha.
11 Kondwerani mwa Yehova inu olungama; imbani, inu nonse amene muli owongoka mtima!
E olioli ia Iehova, a e hauoli, e ka poe pono: E hooho no ka hauoli, e ka poe a pau i kupono ka naau.

< Masalimo 32 >