< Masalimo 31 >
1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Mwa Inu Yehova, ine ndimathawiramo; musalole nʼkomwe kuti ndichititsidwe manyazi; mundipulumutse chifukwa cha chilungamo chanu.
MAING, i liki komui, kom kotin ieiang ia, pwe i ender namenokala kokolata; dore kin ia la duen omui pung.
2 Tcherani khutu lanu kwa ine, bwerani msanga kudzandilanditsa; mukhale thanthwe langa lothawirapo, linga lolimba kundipulumutsa ine.
Kapaikidi dong ia karong ar akan, madang sauasa ia! Kom kotin wiala ai paipalap roson, o kele pa i, pwen sauasa ia!
3 Popeza Inu ndinu thanthwe langa ndi linga langa, chifukwa cha dzina lanu tsogolereni ndi kundiwongolera.
Pwe komui ai paip, o ai kel. Kom kotin kalua ia pweki mar omui.
4 Ndimasuleni mu msampha umene anditchera pakuti ndinu pothawirapo panga.
Kom kotin api ia sang nan insar, me re wiai ong ia, pwe komui kele pa i.
5 Mʼmanja mwanu ndipereka mzimu wanga; womboleni Yehova Mulungu wachoonadi.
I kakaliki ong komui ngen i; kom kotin dore ia la, komui Maing Kot melel.
6 Koma ine ndimadana nawo amene amamamatira mafano achabechabe; ine ndimadalira Yehova.
I suedeki me kin kaporoporeki dikedik en ani mal akan, a i liki Ieowa.
7 Ndidzakondwa ndi kusangalala mʼchikondi chanu popeza Inu munaona masautso anga ndipo mumadziwa kuwawa kwa moyo wanga.
I pan pereperen o polauleki omui kalangan, pwe komui me kotin mangi ai luet, o kotin kupura ngen i ni ansau apwal.
8 Inu simunandipereke kwa mdani koma mwayika mapazi anga pa malo otakasuka.
O re der mueid ong ai imwintiti, ren kaloe ia di. Kom kotin kasone nä i kat nan wasa salatok.
9 Mundichitire chifundo Inu Yehova pakuti ndili pa mavuto; maso anga akulefuka ndi chisoni, mʼmoyo mwanga ndi mʼthupi mwanga momwe mukupweteka.
Ieowa, kom kotin maki ong ia, pwe i masak; mas ai suedelar ki ai mamauk, pil dueta ngen i o pali war ai.
10 Moyo wanga ukunyeka chifukwa cha kuwawidwa mtima ndi zaka zanga chifukwa cha kubuwula; mphamvu zanga zatha chifuwa cha masautso, ndipo mafupa anga akulefuka.
Pwe maur i luet kilar ai insensued, o ai par akan malaulaular ki ai sangesang, ai kelail tikitikelar pweki dip ai, o kokon ai kan luetalar.
11 Chifukwa cha adani anga onse, ndine wonyozeka kwambiri ndi anansi anga; ndine chochititsa manyazi kwa abwenzi anga. Iwo amene amandiona mu msewu amandithawa.
Ai imwintiti kan karos lalaue ia, o i wialar kanamenok pan men imp ai kan, o kamasak pan sau i kan; me kilang ia nani al o, kin tangwei sang ia.
12 Ine ndinayiwalika kwa iwo ngati kuti ndinamwalira; ndakhala ngati mʼphika wosweka.
Aramas monoke ia lar dueta me melar amen; ngai rasong dal eu, me mor pasang.
13 Pakuti ine ndamva zonena zoyipa za anthu ambiri; zoopsa zandizungulira mbali zonse; iwo akukonza chiwembu kuti alimbane nane, kuti atenge moyo wanga.
Pwe i ronger duen me toto kin puserokiong ia; men kamasak kapil ia pena; re kin kapung pena duen ngai, pwen kame ia la.
14 Koma ndikudalira Inu Yehova; ndikunena kuti, “Ndinu Mulungu wanga.”
A i kin kaporoporeki komui Maing, i ap inda: Komui ta ai Kot!
15 Masiku anga ali mʼmanja mwanu; ndipulumutseni kwa adani anga ndi kwa iwo amene akundithamangitsa.
Ai ansau mi nan lim omui, dore ia sang nan pa en ai imwintiti kan o sang me kin pakipaki ia.
16 Walitsani nkhope yanu pa mtumiki wanu; pulumutseni mwa chikondi chanu chosatha.
Kamarainiki sapwilim omui ladu silang omui, dore ia ki omui, dore ia ki omui kalangan.
17 Yehova musalole kuti ndichite manyazi, pakuti ndalirira kwa Inu; koma oyipa achititsidwe manyazi ndipo agone chete mʼmanda. (Sheol )
Maing, kom der kotin mueid ong, i en soredi; pwe i likwiri wong komui. Me sapung kan en soredi, pwe irail en nenenla nan wasan mela. (Sheol )
18 Milomo yawo yabodzayo ikhale chete, pakuti chifukwa cha kunyada ayankhula modzikuza kutsutsana ndi wolungama.
Kil en au en me likam akan en nenenla, irail, me lalaue me pung kan ni laumaum, o aklapalap, o kaurur.
19 Ndi waukulu ubwino wanu umene mwawasungira amene amakuopani, umene mumapereka anthu akuona kwa iwo amene amathawira kwa Inu.
Meid laud omui kalangan, me kom kotin nekinekid ong me lan komui kan, o me kom kin kasale ong ir, me liki komui sansal mon aramas akan.
20 Mu mthunzi wa pamalo popezeka panu muwabisa, kuwateteza ku ziwembu za anthu; mʼmalo anu okhalamo mumawateteza kwa anthu owatsutsa.
Kom kin kotin karir ir ala re omui sang karos, me kailong kin ir; kom kin kadupal ir edi sang mon lo akamai.
21 Matamando akhale kwa Yehova, pakuti anaonetsa chikondi chake chodabwitsa kwa ine pamene ndinali mu mzinda wozingidwa.
Kapinga ong Ieowa, me kotin kalangan laud ong ia nan kanim tengeteng eu.
22 Ndili mʼnkhawa zanga ndinati, “Ine ndachotsedwa pamaso panu!” Komabe Inu munamva kupempha chifundo kwanga pamene ndinapempha thandizo kwa Inu.
Pwe ni ai peikasal i indindar: I lokidokilar sang mon silang ar. Ari so, kom kotin ereki ngil en ai ngidingid, ni ai potoan werwiwer ong komui.
23 Kondani Yehova oyera mtima ake onse! Yehova amasunga wokhulupirika koma amalanga kwathunthu anthu odzikuza.
Komail sapwilim a saraui kan karos, pok ong Ieowa! Ieowa kin kotin sinsila me poson akan, ap depuk ong ir melel, me aklapalap akan.
24 Khalani ndi nyonga ndipo limbani mtima, inu nonse amene mumayembekezera Yehova.
Komail karos me kaporoporeki Ieowa, en kelail o der masak!