< Masalimo 30 >
1 Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba popereka Nyumba ya Mulungu. Ndidzakukwezani Yehova, chifukwa mwanditulutsa kwakuya, ndipo simunalole kuti adani anga akondwere pa ine.
Kathutkung: Devit Oe BAWIPA na pholen han. Bangkongtetpawiteh, na tawmrasang. Ka tarannaw ni na panuikhai hane na pasoung hoeh.
2 Inu Yehova Mulungu wanga ndinapempha kwa Inu thandizo ndipo Inu munandichiritsa.
Oe BAWIPA, ka Cathut, nang koe ka hram teh, na kabawp teh na dam sak.
3 Inu Yehova, munanditulutsa ku manda, munandisunga kuti ndisatsalire mʼdzenje. (Sheol )
Oe BAWIPA, ka hringnae heh phuen thung hoi na rasa teh, tangkom dawk ka bo hoeh nahanlah na hring sak. (Sheol )
4 Imbirani Yehova inu anthu ake okhulupirika; tamandani dzina lake loyera.
A tamikathoungnaw, BAWIPA pholen hoi la sak awh. A min kathoung pahnim hoeh nahanlah, konawm lawk dei awh.
5 Pakuti mkwiyo wake umakhala kwa kanthawi koma kukoma mtima kwake ndi kwa moyo wonse; utha kuchezera kulira usiku wonse, koma chimwemwe chimabwera mmawa.
A lungkhueknae teh tawkkadek doeh, a ngaikhainae teh hringyung hane doeh. Kanae teh tangmin vah a roe. Hatei, amom vah konawmnae a pha.
6 Pamene ndinaona kuti ndili otetezedwa ndinati, “Sindidzagwedezekanso.”
Ka tawnta nateh, ka vout mahoeh toe ka ti.
7 Inu Yehova, pamene munandikomera mtima, munachititsa phiri langa kuyima chilili; koma pamene munabisa nkhope yanu, ndinataya mtima.
BAWIPA na ngaikhainae lahoi, ka mon teh kacaklah na kangdue sak. Na minhmai na hro toteh, ka lungrei a thai.
8 Kwa Inu Yehova ndinayitana; kwa Ambuye ndinapempha chifundo;
Oe BAWIPA nang koe ka hram teh, BAWIPA koe ka kâhei.
9 “Kodi pali phindu lanji powonongeka kwanga ngati nditsikira ku dzenje? Kodi fumbi lidzakutamandani Inu? Kodi lidzalengeza za kukhulupirika kwanu?
Tangkom dawk ka bo toteh, ka thi ni bang hawinae maw a tawn. Vaiphu ni na pholen vaiteh na lawkkatang hah a pâpho han na maw.
10 Imvani Yehova ndipo mundichitire chifundo; Yehova mukhale thandizo langa.”
Oe BAWIPA, ka lawk na thai pouh haw. Na pahren haw. BAWIPA kabawmkung lah pou awm haw.
11 Inu munasandutsa kulira kwanga kukhala kuvina; munachotsa chiguduli changa ndi kundiveka ndi chimwemwe,
Ka cingounae hah lamnae lah na coung sak.
12 kuti mtima wanga uthe kuyimbira Inu usakhale chete. Yehova Mulungu wanga, ndidzapereka kwa Inu mayamiko kwamuyaya.
Apout totouh ka bawilennae ni kâhat laipalah na pholen teh, la a sak thai nahanlah, Oe BAWIPA ka Cathut, a yungyoe hoi konawmnae lawk ka dei han.