< Masalimo 3 >
1 Salimo la Davide. Atathawa mwana wake Abisalomu. Inu Yehova, achulukadi adani anga! Achulukadi amene andiwukira!
Господе! Како је много непријатеља мојих! Многи устају на ме.
2 Ambiri akunena za ine kuti, “Mulungu sadzamupulumutsa.” (Sela)
Многи говоре за душу моју: Нема му помоћи од Бога.
3 Koma Inu Yehova, ndinu chishango chonditeteza, Inu mwandiveka ulemerero ndipo mwanditukula.
Али Ти си, Господе, штит који ме заклања, слава моја; Ти подижеш главу моју.
4 Kwa Yehova, Ine ndilira mofuwula ndipo Iye amandiyankha kuchokera ku phiri lake loyera. (Sela)
Гласом својим вичем ка Господу, и чује ме са свете горе своје.
5 Ine ndimagona ndi kupeza tulo; ndimadzukanso chifukwa Yehova amandichirikiza.
Ја лежем, спавам и устајем, јер ме Господ чува.
6 Sindidzaopa adani anga osawerengeka amene abwera kulimbana nane kuchokera ku madera onse.
Не бојим се много хиљада народа што са свих страна наваљује на ме.
7 Dzukani, Inu Yehova! Pulumutseni, Inu Mulungu wanga. Akantheni adani anga onse pa msagwada; gululani mano a anthu oyipa.
Устани, Господе! Помози ми, Боже мој! Јер Ти удараш по образу све непријатеље моје; разбијаш зубе безбожницима.
8 Chipulumutso chimachokera kwa Yehova. Madalitso akhale pa anthu anu. (Sela)
Од Господа је спасење; нека буде на народу Твом благослов Твој!