< Masalimo 28 >

1 Salimo la Davide. Kwa Inu ine ndiyitana, Yehova ndinu Thanthwe langa; musakhale osamva kwa ine. Pakuti mukapitirira kukhala chete, ndidzakhala ngati iwo amene atsikira ku dzenje.
Доамне, кэтре Тине стриг. Стынка мя! Ну рэмыне сурд ла гласул меу, ка ну кумва, дакэ Те вей депэрта фэрэ сэ-мь рэспунзь, сэ ажунг ка чей че се кобоарэ ын гроапэ!
2 Imvani kupempha chifundo kwanga pomwe ndikuyitana kwa Inu kuti mundithandize, pomwe ndikukweza manja anga kuloza ku malo anu oyeretsetsa.
Аскултэ гласул ругэчунилор меле, кынд стриг кэтре Тине ши кынд ымь ридик мыниле спре Локашул Тэу чел Сфынт!
3 Musandikokere kutali pamodzi ndi anthu oyipa, pamodzi ndi iwo amene amachita zoyipa, amene amayankhula mwachikondi ndi anzawo koma akusunga chiwembu mʼmitima mwawo.
Ну мэ луа де пе пэмынт ымпреунэ ку чей рэй ши ку оамений нелеӂюиць, каре ворбеск де паче апроапелуй лор ши, кынд коло, ау рэутате ын инимэ!
4 Muwabwezere chifukwa cha zochita zawo ndi ntchito zawo zoyipa; abwezereni chifuwa cha zimene manja awo achita ndipo mubweretse pa iwo zimene zowayenera.
Рэсплэтеште-ле дупэ лукрэриле лор ши дупэ рэутатя фаптелор лор, рэсплэтеште-ле дупэ лукраря мынилор лор! Дэ-ле плата каре ли се кувине!
5 Popeza iwowo sakhudzidwa ndi ntchito za Yehova, ndi zimene manja ake anazichita, Iye adzawakhadzula ndipo sadzawathandizanso.
Кэч ей ну яу аминте ла лукрэриле Домнулуй, ла лукраря мынилор Луй. Сэ-й добоаре ши сэ ну-й май скоале!
6 Matamando apite kwa Yehova, popeza Iye wamva kupempha chifundo kwanga.
Бинекувынтат сэ фие Домнул, кэч аскултэ гласул ругэчунилор меле!
7 Yehova ndiye mphamvu yanga ndi chishango changa; mtima wanga umadalira Iye, ndipo Ine ndathandizidwa. Mtima wanga umalumphalumpha chifukwa cha chimwemwe ndipo ndidzayamika Iye mʼnyimbo.
Домнул есте тэрия мя ши скутул меу; ын Ел ми се ынкреде инима ши сунт ажутат. Де ачея ымь есте плинэ де веселие инима ши-Л лауд прин кынтэриле меле.
8 Yehova ndi mphamvu ya anthu ake, linga la chipulumutso kwa wodzozedwa wake.
Домнул есте тэрия попорулуй Сэу, Ел есте Стынка избэвитоаре а унсулуй Сэу.
9 Pulumutsani anthu anu ndipo mudalitse cholowa chanu; mukhale mʼbusa wawo ndipo muwakweze kwamuyaya.
Мынтуеште, Доамне, попорул Тэу ши бинекувынтязэ моштениря Та! Фий пэсторул ши сприжиниторул лор ын вечь!

< Masalimo 28 >