< Masalimo 25 >

1 Salimo la Davide. Kwa Inu Yehova, ndipereka moyo wanga.
O Pakai, kahinkho hi nang kapetai.
2 Ndimadalira Inu Mulungu wanga. Musalole kuti ndichite manyazi kapena kuti adani anga andipambane.
Nang katahsan e ka Pathen! Nei jumso hihbeh in, chule kalel na a hin ka melmate kichoisangsah hihbeh in.
3 Aliyense amene amayembekezera kwa Ambuye sadzachititsidwa manyazi koma achinyengo ndiwo adzachititsidwe manyazi ndipo sadzakhala ndi chodzitetezera.
Nangma tahsan koimachan jumna ato loudiu ahi, amavang mijoulhep gojing honvang jumna ato diu ahi.
4 Ndidziwitseni njira zanu Inu Yehova, phunzitseni mayendedwe anu;
O Pakai lamdih chu neihil in; kajuiding lampi chu neikomu peh in.
5 tsogolereni mʼchoonadi chanu ndi kundiphunzitsa, pakuti Inu ndinu Mulungu mpulumutsi wanga, ndipo chiyembekezo changa chili mwa Inu tsiku lonse.
Nathutah chu neihil in hichea chun neipui in ajeh chu nangmahi eihuh hinga ka Pathen chu nahi. Nilhum kei keijin nanga hin kinepna kanei jinge.
6 Kumbukirani Inu Yehova chifundo ndi chikondi chanu chachikulu, pakuti ndi zakalekale.
O Pakai golui a patna neihin puinao nami khoto nale namingailutna longlou hingeldoh in.
7 Musakumbukire machimo a ubwana wanga ndi makhalidwe anga owukira; molingana ndi chikondi chanu ndikumbukireni ine, pakuti Inu Yehova ndinu wabwino.
Kakhangdon lai a kachonset gitlou naho neigeldoh peh hih inlang nami ngailutna longlouva neipuina johchu galdoh in, ajeh chu nangma milungset them nahi, O Pakai.
8 Yehova ndi wabwino ndi wolungama; choncho Iye akulangiza ochimwa mʼnjira yake.
Pakaihi apha ahin adih jengbou abol'e, aman lamdihlouvache hojeng jong lamdih akopeh jinge.
9 Amatsogolera odzichepetsa kuti achite zolungama ndipo amawaphunzitsa njira zake.
Aman mi kineosah hochu lamdih a apuijin ama dei lampi chu ahil jinge.
10 Njira zonse za Yehova ndi zachikondi ndi zokhulupirika kwa iwo amene amasunga zofuna za pangano lake.
Pakai kitepna nitjing holeh ama deipeh dungjuija chonho chu ami ngailutna longlou leh akitahna in apuihoi jinge.
11 Chifukwa cha dzina lanu, Inu Yehova, khululukireni mphulupulu zanga, ngakhale kuti ndi zochuluka.
Namin loupina dingin O Pakai, kachonsetna simjoulou neingai dam in.
12 Tsono ndani munthu amene amaopa Yehova? Yehova adzamulangiza njira yoti ayitsate.
Pakaiging ho chu koi ho hiuvam? Amaho chenading lampi chu Pakai in avetsah ding ahi.
13 Iye adzakhala pa ulemerero masiku ake onse, ndipo zidzukulu zake zidzalandira dziko ngati cholowa chawo.
Amaho chu khangtou untin achateovin jong gamsung alodingu ahi.
14 Yehova amawulula chinsinsi chake kwa iwo amene amamuopa; amawulula pangano lake kwa iwowo.
Pakai hi ama gingjing tedinga golphapen ahin, Aman hitobang miho chu akitepna ahiljing e.
15 Maso anga ali pa Yehova nthawi zonse, pakuti ndi Iye yekha amene adzawonjola mapazi anga mu msampha.
Kamit tenin Pakaichu avejingin, aman kagalmite thangkul a kon in eihuhdoh jinging e.
16 Tembenukirani kwa ine ndipo mundikomere mtima, pakuti ndili ndekhandekha ndipo ndikuzunzika.
Neihin ang-ngatnin lang neikho ton, ajeh chu keima kachangseh a lungthom haotah a uma kahi.
17 Masautso a mu mtima mwanga achulukirachulukira; masuleni ku zowawa zanga.
Kaboi na ho akhoh se cheh un. Oh hichehoa konhin neihuhdoh in.
18 Penyani mazunzo anga ndi zovuta zanga ndipo mufafanize machimo anga onse.
Kalung gimnahi neihet pehin chuleh kahah satna hohi neivet peh inlang kachonset naho ngaidam in.
19 Onani mmene adani anga achulukira ndi momwe chidani chawo ndi ine chakulira.
Ven galmi ijat mong mong kanei hitam chule amahohin ichangeiya eihotnu hitam!
20 Tetezani moyo wanga ndi kundilanditsa; musalole kuti ndichite manyazi, pakuti ndimathawira kwa Inu.
Neivengbit in! amaho akon hin kahinkho huhdoh in! nangma a kisel kahi neijumso hihbeh in.
21 Kukhulupirika ndi kulungama kwanga kunditeteze, chifukwa chiyembekezo changa chili mwa Inu.
Kitah nale thenna in eivengbit hen ajeh chu nanga hin kakinepna aum jinge.
22 Wombolani Israeli Inu Mulungu, ku mavuto ake onse!
Vo Pathen Israelte hi aboi najouseu vakon in lhatdoh tan.

< Masalimo 25 >