< Masalimo 23 >

1 Salimo la Davide. Yehova ndiye mʼbusa wanga, sindidzasowa kanthu.
Господ је пастир мој, ништа ми неће недостајати.
2 Amandigoneka pa msipu wobiriwira, amanditsogolera ku madzi akumwa abwino,
На зеленој паши пасе ме, води ме на тиху воду.
3 amatsitsimutsa moyo wanga. Amanditsogolera mʼnjira zachilungamo chifukwa cha dzina lake.
Душу моју опоравља, води ме стазама праведним имена ради свог.
4 Ngakhale ndiyende mʼchigwa cha mdima wakuda bii, sindidzaopa choyipa, pakuti Inu muli ndi ine; chibonga chanu ndi ndodo yanu zimanditonthoza.
Да пођем и долином сена смртнога, нећу се бојати зла; јер си Ти са мном; штап Твој и палица Твоја теши ме.
5 Mumandikonzera chakudya adani anga akuona. Mumadzoza mutu wanga ndi mafuta; chikho changa chimasefukira.
Поставио си преда мном трпезу на видику непријатељима мојим; намазао си уљем главу моју, и чаша је моја препуна.
6 Zoonadi, zokoma ndi chikondi chosasinthika zidzanditsata masiku onse a moyo wanga, ndipo ndidzakhala mʼNyumba ya Yehova kwamuyaya.
Да! Доброта и милост Твоја пратиће ме у све дане живота мог, и ја ћу наставати у дому Господњем задуго.

< Masalimo 23 >