< Masalimo 23 >

1 Salimo la Davide. Yehova ndiye mʼbusa wanga, sindidzasowa kanthu.
IEOWA sile pa i, i sota pan anane meakot.
2 Amandigoneka pa msipu wobiriwira, amanditsogolera ku madzi akumwa abwino,
A kotin kamanga ia nan mos kaselel o kalua ia wong ni pil lamelamur.
3 amatsitsimutsa moyo wanga. Amanditsogolera mʼnjira zachilungamo chifukwa cha dzina lake.
A kotin kamanada ngen i, a kalua ia pon al pung pweki mar a.
4 Ngakhale ndiyende mʼchigwa cha mdima wakuda bii, sindidzaopa choyipa, pakuti Inu muli ndi ine; chibonga chanu ndi ndodo yanu zimanditonthoza.
I lao weid nan mot en mela, i sota pan masak mesued kot, pwe kom kotin ieiang ia, omui irar o lepin saipali kamait ia la.
5 Mumandikonzera chakudya adani anga akuona. Mumadzoza mutu wanga ndi mafuta; chikho changa chimasefukira.
Kom kotin kaonop dang ia tepel eu salong ai imwintiti kan. Kom kotin keiekidi mong ai le, o ai dal kin wudewudok.
6 Zoonadi, zokoma ndi chikondi chosasinthika zidzanditsata masiku onse a moyo wanga, ndipo ndidzakhala mʼNyumba ya Yehova kwamuyaya.
Pai o kalangan pan idauen ia arain ai maur, o i pan mimieta nan tanpas en Ieowa kokolata.

< Masalimo 23 >