< Masalimo 23 >

1 Salimo la Davide. Yehova ndiye mʼbusa wanga, sindidzasowa kanthu.
Mpiarak’ ahy t’Iehovà, tsy hieran-draho;
2 Amandigoneka pa msipu wobiriwira, amanditsogolera ku madzi akumwa abwino,
Ampandrea’e an-dovoke maindoñe ao, tehafe’e mb’añ’olon-drano mipendreñe mb’eo.
3 amatsitsimutsa moyo wanga. Amanditsogolera mʼnjira zachilungamo chifukwa cha dzina lake.
Vaòe’e ty fiaiko, iaoloa’e mb’an-dalam-bantañe, ty amy tahina’ey.
4 Ngakhale ndiyende mʼchigwa cha mdima wakuda bii, sindidzaopa choyipa, pakuti Inu muli ndi ine; chibonga chanu ndi ndodo yanu zimanditonthoza.
Ndra t’ie miranga i vatanen- talinjon-kavilasiy, tsy ho hemban-karatiañe amy te Ihe ro amako; mpañohò ahiko ty kobai’o naho ty fitoño’o.
5 Mumandikonzera chakudya adani anga akuona. Mumadzoza mutu wanga ndi mafuta; chikho changa chimasefukira.
Halànkañe’o fandambañañe aoloko añatrefan-drafelahiko eo; añiliña’o solike ty lohako, mandopatse ty fitoviko.
6 Zoonadi, zokoma ndi chikondi chosasinthika zidzanditsata masiku onse a moyo wanga, ndipo ndidzakhala mʼNyumba ya Yehova kwamuyaya.
Toe hañorik’ ahy amo hene andro hivelomakoo ty hasoa naho ty fiferenaiñañe; le hitobok’ añ’anjomba’ Iehovà ao nainai’e.

< Masalimo 23 >