< Masalimo 23 >

1 Salimo la Davide. Yehova ndiye mʼbusa wanga, sindidzasowa kanthu.
Hina Gode da na sibi ouligisu dunu. Na da hahanidafa hame esalumu.
2 Amandigoneka pa msipu wobiriwira, amanditsogolera ku madzi akumwa abwino,
E da na gisi nasegagi amo da: iya helefimusa: , oule ahoa.
3 amatsitsimutsa moyo wanga. Amanditsogolera mʼnjira zachilungamo chifukwa cha dzina lake.
E da nama gasa gaheabolo iaha. E da nama ilegele sia: i defele, esalusu logo moloidafa amoga na oule ahoa.
4 Ngakhale ndiyende mʼchigwa cha mdima wakuda bii, sindidzaopa choyipa, pakuti Inu muli ndi ine; chibonga chanu ndi ndodo yanu zimanditonthoza.
Hina Gode! Na da bogosu gasidunasi amo ganodini ahoasea, na da hame beda: mu. Bai Di ani gilisili esalebeba: le. Dia sibi ouligisu galiamo da na gaga: lala.
5 Mumandikonzera chakudya adani anga akuona. Mumadzoza mutu wanga ndi mafuta; chikho changa chimasefukira.
Dia nagili lolo nasu hamonana. Na ha lai dunu ilia ba: ma: ne, Di hamonana. Di nama yosia: ne, nama hahawane nodone aowasa. Di da na faigelei nabalesilala.
6 Zoonadi, zokoma ndi chikondi chosasinthika zidzanditsata masiku onse a moyo wanga, ndipo ndidzakhala mʼNyumba ya Yehova kwamuyaya.
Na dawa: Dia asigi hou amola noga: idafa hou da eso huluane na esalea, nama dialumu. Amola na da Dia diasu ganodini Fifi ahoanusu ba: mu.

< Masalimo 23 >