< Masalimo 21 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Inu Yehova, mfumu ikusangalala mu mphamvu yanu, chimwemwe chake nʼchachikuludi pa kupambana kumene mumapereka!
O Jeova, gui minetgotmo ninamagof y ray; ya gui satbasionmo ninamagof megae!
2 Inu mwayipatsa zokhumba za mtima wake ndipo simunayimane zopempha za pa milomo yake. (Sela)
Y minalago y corasonña, jago numae: ya ti unpune ni y guinagao y labiosña.
3 Inu munayilandira ndi madalitso ochuluka ndipo munayiveka chipewa chaufumu chagolide weniweni pa mutu wake.
Sa untagam güe nu y bendision y minauleg: y coronan oro nu y fino, unpolo gui jilo y iluña.
4 Iye anakupemphani moyo, ndipo munamupatsa masiku ochuluka kwamuyaya.
Linâlâ na guinagaoña unnae: y anaco na jaane, para siempre taejinecog.
5 Kudzera mʼzigonjetso zimene munapereka, ulemerero wake ndi waukulu; Inu mwapereka pa iyo ulemerero ndi ufumu.
Dangculo y minalagña gui satbasionmo: onra yan minagas unpolo gui jiloña.
6 Zoonadi Inu mwayipatsa madalitso amuyaya, Inu mwayipatsa chisangalalo ndi chimwemwe chimene chili pamaso panu.
Sa jago bumendise para taejinecog: unnamagof güe yan minagof gui menamo.
7 Pakuti mfumu imadalira Yehova; kudzera mʼchikondi chake chosatha cha Wammwambamwamba, iyo sidzagwedezeka.
Sa y ray jaangongoco si Jeova: ya pot y minaase y Gueftaquilo ti calamten.
8 Dzanja lanu lidzayimitsa adani anu onse; dzanja lanu lamanja lidzagwira adani anu.
Y canaemo usoda todo y enimigumo: y agapa na canaemo usoda todo y chumatlie jao.
9 Pa nthawi ya kuonekera kwanu mudzawasandutsa ngʼanjo yamoto yotentha. Mu ukali wake Yehova adzawameza, ndipo moto wake udzawatha.
Jago pumolo sija taegüije y jetnon guafe gui tiempon binibumo: si Jeova yumulang sija anae lalalo, ya y guafe ufanlinachae.
10 Inu mudzawononga ana awo pa dziko lapansi, zidzukulu zawo pakati pa anthu.
Ya y tinegchaña unyulang gui jilo y tano, ya y semiyaña gui entalo y famaguon y taotao.
11 Ngakhale iwo akukonzereni chiwembu mwa kuchenjera kwawo sadzapambana;
Sa jagasja majasuye y taelaye contra jago: jagasja majaso y dinague ni y ti siña mafatinas.
12 pakuti mudzawapirikitsa ndipo adzaonetsa misana yawo pamene mudzawaloza ndi mivi yanu.
Sa jago fumatinas na jabira y tataloñija ya unnalisto y jalon y atcosmo contra y matañija.
13 Mukwezeke Inu Yehova mʼmphamvu yanu, ife tidzayimba nyimbo ndi kutamanda mphamvu yanu.
Taquilo jao, O Jeova, yan y minetgotmo: incantaye yan inalabaye y ninasiñamo.

< Masalimo 21 >