< Masalimo 20 >

1 Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Yehova akuyankhe pamene uli pa msautso; dzina la Mulungu wa Yakobo likuteteze.
Davidin Psalmi, edelläveisaajalle. Herra kuulkoon sinua hädässäs, Jakobin Jumalan nimi sinua varjelkoon!
2 Iye atumize thandizo kuchokera ku malo ake opatulika; akugwirizize kuchokera ku Ziyoni.
Hän lähettäköön sinulle apua pyhästä ja Zionista sinua vahvistakoon!
3 Iye akumbukire nsembe zako zonse ndipo alandire nsembe zako zopsereza. (Sela)
Hän muistakoon kaikki ruokauhris, ja sinun polttouhris olkoon lihavat, (Sela)
4 Akupatse chokhumba cha mtima wako ndipo akuthandize kuti zonse wakonza zichitike.
Hän antakoon sinulle, mitä sinun sydämes anoo, ja päättäköön kaikki aivoitukses!
5 Ife tidzafuwula ndi chimwemwe pamene iwe wapambana ndipo tidzanyamula mbendera zathu mʼdzina la Mulungu wathu, Yehova ayankhe zopempha zako zonse.
Me kerskaamme sinun avustas, ja meidän Jumalamme nimessä me ylennämme lippumme: Herra täyttäköön kaikki sinun rukoukses!
6 Tsopano ndadziwa kuti Yehova amapulumutsa wodzozedwa wake; Iye amamuyankha kuchokera kumwamba ku malo ake opatulika ndi mphamvu yopulumutsa ya dzanja lake lamanja.
Nyt minä tunnen Herran voideltuansa auttavan, ja häntä kuulevan pyhästä taivaastansa: hänen oikia kätensä auttaa voimallisesti.
7 Ena amadalira magaleta ndipo ena akavalo koma ife tidzadalira dzina la Yehova Mulungu wathu.
Nämät uskaltavat rattaisiin ja oreihin; mutta me muistamme Herran Jumalamme nimeä.
8 Iwo amagonjetsedwa ndi kugwa, koma ife timadzuka ndi kuyima chilili.
He ovat kukistetut ja langenneet; mutta me nousemme ja pystyällä seisomme.
9 Inu Yehova, pulumutsani mfumu! Tiyankheni pamene tikuyitanani!
Auta Herra! Kuningas meitä kuulkaan, kuin me huudamme.

< Masalimo 20 >