< Masalimo 2 >

1 Nʼchifukwa chiyani anthu a mitundu ina akufuna kuchita chiwembu? Akonzekeranji zopanda pake anthu?
Adɛn nti na amanaman no hyehyɛ bɔne ho na nnipa no bɔ pɔw hunu yi?
2 Mafumu a dziko lapansi akugwirizana nazo; ndipo olamulira asonkhana pamodzi kulimbana ndi Ambuye ndi wodzozedwa wakeyo.
Asase so ahemfo sɔre gyina na sodifo ka wɔn ho bɔ mu tia Awurade ne Nea Wɔasra no no.
3 Iwo akunena kuti, “Tiyeni timasule magoli awo ndipo titaye zingwe zawo.”
Wɔka se, “Momma yemmubu wɔn nkɔnsɔnkɔnsɔn na yɛntow wɔn mpokyerɛ ngu.”
4 Wokhala mmwamba akuseka; Ambuye akuwanyoza iwowo.
Nea ɔte agua so wɔ ɔsoro no serew; Awurade di wɔn ho fɛw.
5 Ndipo iye awadzudzula mu mkwiyo wake ndi kuwaopseza mu ukali wake, kunena kuti,
Afei ɔka wɔn anim wɔ nʼabufuw mu, hunahuna wɔn wɔ nʼabufuwhyew mu, ka se,
6 “Ine ndakhazikitsa mfumu yanga pa Ziyoni, phiri langa loyera.”
“Masi me Hene wɔ Sion, me bepɔw kronkron no so.”
7 Ine ndidzalengeza zimene Yehova walamula: Iye anati kwa Ine, “Iwe ndiwe mwana wanga; lero Ine ndakhala Atate ako.
Mɛpae mu aka Awurade ahyɛde: Ɔka kyerɛɛ me se, “Woyɛ me Ba; nnɛ mayɛ wʼAgya.
8 Tandipempha, ndipo ndidzachititsa kuti mitundu ya anthu ikhale cholowa chako; malekezero a dziko lapansi kuti akhale chuma chako.
Bisa me, na mede amanaman nyinaa bɛyɛ wʼagyapade, asase ano nyinaa bɛyɛ wo de.
9 Iweyo udzawalamulira ndi ndodo yaufumu yachitsulo; udzawaphwanya zidutswazidutswa ngati zowumba zadothi.”
Wode dade ahempema bedi wɔn so; na woabobɔ wɔn sɛ ɔnwemfo ahina.”
10 Kotero, inu mafumu, chenjerani; chenjezedwani, inu olamulira a dziko lapansi.
Enti mo ahemfo, munsua nyansa; monkae kɔkɔbɔ yi, mo asase sodifo.
11 Tumikirani Yehova mwa mantha ndi kukondwerera ulamuliro wake monjenjemera.
Momfa osuro nsom Awurade na monsɛpɛw mo ho ahopopo mu.
12 Mpsopsoneni mwanayo kuti angakwiye; kuti mungawonongedwe mʼnjira zanu, pakuti ukali wake utha kuuka mʼkanthawi kochepa. Odala ndi onse amene amathawira kwa Iye.
Mumfew Ɔba no ano, na ne bo amfuw na mo akwan de mo bɛkɔ ɔsɛe mu, efisɛ nʼabufuwhyew tumi sɔre mpofirim. Nhyira ne wɔn a woguan toa no nyinaa.

< Masalimo 2 >