< Masalimo 2 >

1 Nʼchifukwa chiyani anthu a mitundu ina akufuna kuchita chiwembu? Akonzekeranji zopanda pake anthu?
Ino ty fidabasida’ o kilakila ondatio, naho ty fikililia’ ondatio raha tsy vente’e.
2 Mafumu a dziko lapansi akugwirizana nazo; ndipo olamulira asonkhana pamodzi kulimbana ndi Ambuye ndi wodzozedwa wakeyo.
Mijohañe o mpanjaka’ ty tane toio, naho mitrao-kinia o mpifeheo hiatreatre am’ Iehovà naho i Noriza’ey, manao ty hoe:
3 Iwo akunena kuti, “Tiyeni timasule magoli awo ndipo titaye zingwe zawo.”
Antao handrafadrafatse o talirandra’ iareoo, le hahimpan-tika o rohi’ iareoo.
4 Wokhala mmwamba akuseka; Ambuye akuwanyoza iwowo.
Miankahake i mpiambesatse an-dindiñey; mitsikìke iareo t’i Talè.
5 Ndipo iye awadzudzula mu mkwiyo wake ndi kuwaopseza mu ukali wake, kunena kuti,
Fa ho trevohe’e an-keloke, vaho hampinevenevere’e am-pifombo’e:
6 “Ine ndakhazikitsa mfumu yanga pa Ziyoni, phiri langa loyera.”
Toe izaho ty nañoriñe ty Mpanjakako e Tsiône ao amy vohiko miavakey.
7 Ine ndidzalengeza zimene Yehova walamula: Iye anati kwa Ine, “Iwe ndiwe mwana wanga; lero Ine ndakhala Atate ako.
Sokireko ho lily: hoe t’Iehovà amako: Anako irehe, anindroany ty nampiareñako azo.
8 Tandipempha, ndipo ndidzachititsa kuti mitundu ya anthu ikhale cholowa chako; malekezero a dziko lapansi kuti akhale chuma chako.
Mihalalia amako le hampandovaeko Azo o fifeheañeo, naho ho fanaña’o o olon-taneo.
9 Iweyo udzawalamulira ndi ndodo yaufumu yachitsulo; udzawaphwanya zidutswazidutswa ngati zowumba zadothi.”
Ho pozahe’o am-bodam-by; Hampijeñajeñahe’e hoe siniharam-panao valàñe-tane.
10 Kotero, inu mafumu, chenjerani; chenjezedwani, inu olamulira a dziko lapansi.
Aa le mahihira ry mpanjakao; Mimetea oke ry mpizaka’ ty tane toio.
11 Tumikirani Yehova mwa mantha ndi kukondwerera ulamuliro wake monjenjemera.
Toroño am-pañeveñañe t’Iehovà, vaho mirebeha am-pineveneverañe;
12 Mpsopsoneni mwanayo kuti angakwiye; kuti mungawonongedwe mʼnjira zanu, pakuti ukali wake utha kuuka mʼkanthawi kochepa. Odala ndi onse amene amathawira kwa Iye.
Ondroho i Anakey tsy mone hiviñera’e, vaho hihomak’ an-dalañe ey nahareo; fa mete hisolebatse aniany ty fifombo’e. Hene haha ze mitsolok’ ama’e.

< Masalimo 2 >