< Masalimo 2 >

1 Nʼchifukwa chiyani anthu a mitundu ina akufuna kuchita chiwembu? Akonzekeranji zopanda pake anthu?
Apay nga agrebelde dagiti nasion, ken agtutulag dagiti tattao iti awan serserbina?
2 Mafumu a dziko lapansi akugwirizana nazo; ndipo olamulira asonkhana pamodzi kulimbana ndi Ambuye ndi wodzozedwa wakeyo.
Agkaykaysa nga agsagana dagiti ari iti daga ken agkaykaysa dagiti mangiturturay nga agtutulag a maibusor kenni Yahweh ken iti Mesiasna, a kunada,
3 Iwo akunena kuti, “Tiyeni timasule magoli awo ndipo titaye zingwe zawo.”
“Pugsatentayo dagiti posas nga inkabilda kadatayo ken ibellengtayo dagiti kawarda.”
4 Wokhala mmwamba akuseka; Ambuye akuwanyoza iwowo.
Isuna a nakatugaw kadagiti langit, uyawennanto ida; lalaisen ti Apo ida.
5 Ndipo iye awadzudzula mu mkwiyo wake ndi kuwaopseza mu ukali wake, kunena kuti,
Ket agsao isuna kadakuada iti ungetna ken butbutngenna ida iti pungtotna, a kunana,
6 “Ine ndakhazikitsa mfumu yanga pa Ziyoni, phiri langa loyera.”
Siak a mismo ti nangpulot iti arik idiay Sion, ti nasantoan a bantayko.”
7 Ine ndidzalengeza zimene Yehova walamula: Iye anati kwa Ine, “Iwe ndiwe mwana wanga; lero Ine ndakhala Atate ako.
Ipakaammokto ti bilin ni Yahweh. Kinunana kaniak, “Sika ti anakko! Ita nga aldaw, nagbalinak nga amam.
8 Tandipempha, ndipo ndidzachititsa kuti mitundu ya anthu ikhale cholowa chako; malekezero a dziko lapansi kuti akhale chuma chako.
Agkiddawka kaniak, ket itedko kenka dagiti nasion a tawidmo ken dagiti kaadaywan a rehion iti daga a sanikuam.
9 Iweyo udzawalamulira ndi ndodo yaufumu yachitsulo; udzawaphwanya zidutswazidutswa ngati zowumba zadothi.”
Burakemto ida babaen iti setro a landok; rumekemto ida a kasla banga ti agdamdamili.”
10 Kotero, inu mafumu, chenjerani; chenjezedwani, inu olamulira a dziko lapansi.
Isu nga ita, dakayo nga ari, maballaagankayo; masuroankayo, dakayo a mangiturturay iti daga.
11 Tumikirani Yehova mwa mantha ndi kukondwerera ulamuliro wake monjenjemera.
Dayawenyo ni Yahweh nga addaan panagbuteng ken agrag-okayo nga addaan panagpigerger.
12 Mpsopsoneni mwanayo kuti angakwiye; kuti mungawonongedwe mʼnjira zanu, pakuti ukali wake utha kuuka mʼkanthawi kochepa. Odala ndi onse amene amathawira kwa Iye.
Agkanyo ti anak amangan no makaungetto isuna kadakayo, ket mataykayo iti dalan inton dagus a sumged ti ungetna. Anian a nagasat dagiti amin nga agkamang kenkuana.

< Masalimo 2 >