< Masalimo 2 >
1 Nʼchifukwa chiyani anthu a mitundu ina akufuna kuchita chiwembu? Akonzekeranji zopanda pake anthu?
Hvorfor fnyser Hedninger, hvi pønser Folkefærd paa, hvad faafængt er?
2 Mafumu a dziko lapansi akugwirizana nazo; ndipo olamulira asonkhana pamodzi kulimbana ndi Ambuye ndi wodzozedwa wakeyo.
Jordens Konger rejser sig, Fyrster samles til Raad mod HERREN og mod hans Salvede:
3 Iwo akunena kuti, “Tiyeni timasule magoli awo ndipo titaye zingwe zawo.”
»Lad os sprænge deres Baand og kaste Rebene af os!«
4 Wokhala mmwamba akuseka; Ambuye akuwanyoza iwowo.
Han, som troner i Himlen, ler, Herren, han spotter dem.
5 Ndipo iye awadzudzula mu mkwiyo wake ndi kuwaopseza mu ukali wake, kunena kuti,
Saa taler han til dem i Vrede, forfærder dem i sin Harme:
6 “Ine ndakhazikitsa mfumu yanga pa Ziyoni, phiri langa loyera.”
»Jeg har dog indsat min Konge paa Zion, mit hellige Bjerg!«
7 Ine ndidzalengeza zimene Yehova walamula: Iye anati kwa Ine, “Iwe ndiwe mwana wanga; lero Ine ndakhala Atate ako.
Jeg kundgør HERRENS Tilsagn. Han sagde til mig: »Du er min Søn, jeg har født dig i Dag!
8 Tandipempha, ndipo ndidzachititsa kuti mitundu ya anthu ikhale cholowa chako; malekezero a dziko lapansi kuti akhale chuma chako.
Bed mig, og jeg giver dig Hedningefolk til Arv og den vide Jord i Eje;
9 Iweyo udzawalamulira ndi ndodo yaufumu yachitsulo; udzawaphwanya zidutswazidutswa ngati zowumba zadothi.”
med Jernspir skal du knuse dem og sønderslaa dem som en Pottemagers Kar!«
10 Kotero, inu mafumu, chenjerani; chenjezedwani, inu olamulira a dziko lapansi.
Og nu, I Konger, vær kloge, lad eder raade, I Jordens Dommere,
11 Tumikirani Yehova mwa mantha ndi kukondwerera ulamuliro wake monjenjemera.
tjener HERREN i Frygt, fryd jer med Bæven!
12 Mpsopsoneni mwanayo kuti angakwiye; kuti mungawonongedwe mʼnjira zanu, pakuti ukali wake utha kuuka mʼkanthawi kochepa. Odala ndi onse amene amathawira kwa Iye.
Kysser Sønnen, at ikke han vredes og I forgaar! Snart blusser hans Vrede op. Salig hver den, der lider paa ham!