< Masalimo 17 >

1 Pemphero la Davide. Imvani Inu Yehova pempho langa lachilungamo; mverani kulira kwanga. Tcherani khutu kuti mumve pemphero langa popeza silikuchokera pakamwa pachinyengo.
Kathutkung: Devit Oe BAWIPA, lannae koe lah awm nateh, ka hramnae hah na thai pouh haw. Dumnae ka dei boihoeh e pahni hoi ka ratoumnae hah na thai pouh haw.
2 Kusalakwa kwanga kuchokera kwa inu; maso anu aone chimene ndi cholungama.
Ka kong dawk lawk tâtuengnae hah na hmalah tâcawt naseh, na mit teh kalan e hno dawk um naseh.
3 Ngakhale Inu mutafufuza mtima wanga ndi kundisanthula usiku, ngakhale mutandiyesa, simudzapeza kanthu; Ine ndatsimikiza kuti pakamwa panga sipadzachimwa.
Ka lungthin teh na tanouk toe. Karum vah na pai toe. Na tanouk teh banghai na hmawt hoeh. Ka pahni ni payon hoeh nahanelah ka noe toe.
4 Kunena za ntchito za anthu, monga mwa mawu a pakamwa panu, Ine ndadzisunga ndekha posatsata njira zachiwawa.
Taminaw ni sak e kong dawk, karaphoekungnaw e lam hah na lawk lahoi ouk ka roun toe.
5 Mayendedwe anga akhazikika pa njira zanu; mapazi anga sanaterereke.
Na lamthung dawk ka dawn lahun nah ka tâlaw payon hoeh nahanlah, na ka bawm haw.
6 Ine ndikuyitana Inu, Mulungu wanga, pakuti mudzandiyankha; tcherani khutu lanu kwa ine ndipo mumve pemphero langa.
Oe Cathut, nang ni na thai pouh dawkvah, kai ni ka hei. Na hnâ pakeng nateh, ka lawk hah na thai pouh haw.
7 Onetsani kudabwitsa kwa chikondi chanu chachikulu, Inu amene mumapulumutsa ndi dzanja lanu lamanja iwo amene amathawira kwa inu kuchoka kwa adani awo.
Nang kâuepnaw hah, katarankungnaw e kut dawk hoi, rungngangkung Cathut, pahrenlungmanae hah kamnuek sak haw.
8 Mundisunge ine ngati mwanadiso; mundibise mu mthunzi wa mapiko anu,
Kai rep na kacuengroe e tamikayonnaw hoi kai thei hanlah na kalup e tarannaw kut dawk hoi,
9 kuchoka kwa oyipa amene amandizinga ine, kuchoka kwa anthu amene ndi adani anga, amene andizungulira ine.
Mitmu patetlah kai hah na ring haw. Na rathei rahim vah na ramuk haw.
10 Iwo amatseka mitima yawo yopanda chifundo, ndi pakamwa pawo amayankhula modzitamandira.
Ahnimouh teh amamae thâwnae hah a kâuep awh teh, kâoup laihoi lawk a dei awh.
11 Andisaka, tsopano andizungulira ndi maso awo atcheru, kuti andigwetse pansi.
Ka ceinae lam hah a kalup awh teh, talai dawk rawp sak hanelah a mit pakhap laipalah na khet awh.
12 Iwo ali ngati mkango wofuna nyama; ngati mkango waukulu wokhala mobisala.
Sendek ni a kei e moi ca han thouk a ngai e patetlah thoseh, sendek kanaw ni arulahoi a pawp e patetlah thoseh ao awh.
13 Dzukani Yehova, mulimbane nawo ndipo muwagwetse pansi; landitseni kuchoka kwa oyipa ndi lupanga lanu.
Oe BAWIPA, thaw haw. Kangdout sin nateh, rawm sak haw. Tamikathoutnaw e kut dawk hoi na tahloi hoi na rungngang haw.
14 Inu Yehova, pulumutseni ndi dzanja lanu kwa anthu otere, kwa anthu a dziko lino amene mphotho yawo ili mʼmoyo uno. Inu mumaletsa njala kwa amene asangalatsidwa nanu; ana awo aamuna ali ndi zinthu zambiri, ndipo iwo amasunga chuma cha ana awo.
Oe BAWIPA, talai tami lah kaawm e hotnaw e kut dawk hoi na rungngang haw. Ahnimouh teh atuvah, amamouh hanelah, a pang awh toe. Ahnimae ngainae hah hnopai hoi a kawi sak. A canaw hai a tawnta awh teh, a catounnaw koe a hnopainaw hah a parâw pouh awh.
15 Ndipo ine mʼchilungamo ndidzaona nkhope yanu; pamene ndidzadzuka, ndidzakondwera kwambiri poonana nanu.
Kai niteh, lannae lahoi na minhmai ka hmu han. Nang patetlah ka kâhlaw toteh ka lung a kuep han.

< Masalimo 17 >