< Masalimo 16 >

1 Mikitamu ya Davide. Ndisungeni Inu Mulungu, pakuti ine ndimathawira kwa Inu.
Ett gyldene klenodium Davids. Bevara mig, Gud; förty jag tröstar uppå dig.
2 Ndinati kwa Yehova, “Inu ndinu Ambuye anga; popanda Inu, ine ndilibe chinthu chinanso chabwino.”
Jag hafver sagt till Herran: Du äst ju Herren; jag måste för dina skull lida.
3 Kunena za oyera mtima amene ali pa dziko, amenewa ndi olemekezeka, amene ndimakondwera nawo.
För de heliga, som på jordene äro, och för de härliga, till dem hafver jag allt mitt behag.
4 Anthu amene amathamangira kwa milungu ina mavuto awo adzachulukadi. Ine sindidzathira nawo nsembe zawo zamagazi kapena kutchula mayina awo ndi pakamwa panga.
Men de som efter en annan löpa, skola stor bedröfvelse hafva; jag vill icke offra deras drickoffer med blod, eller föra deras namn i minom mun.
5 Yehova, Inu mwandipatsa cholowa changa ndi chikho changa; mwateteza kolimba gawo langa.
Men Herren är mitt gods och min del; du uppehåller min arfvedel.
6 Malire a malo anga akhala pabwino; ndithudi, ine ndili cholowa chokondweretsa kwambiri.
Lotten är mig fallen i det lustiga; mig är en skön arfvedel tillfallen.
7 Ine ndidzatamanda Yehova amene amandipatsa uphungu; ngakhale usiku mtima wanga umandilangiza.
Jag lofvar Herran, den mig råd gifvit hafver; tukta mig också mine njurar om nattena.
8 Ndayika Yehova patsogolo panga nthawi zonse. Popeza Iyeyo ali kudzanja langa lamanja, sindidzagwedezeka.
Jag hafver Herran för ögon alltid: ty han är mig på högra handene; derföre skall jag väl blifva vid mig.
9 Choncho mtima wanga ndi wosangalala ndipo pakamwa panga pakukondwera; thupi langanso lidzakhala pabwino,
Derföre gläder sig mitt hjerta, och min ära är glad, och mitt kött skall säkert ligga.
10 chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. (Sheol h7585)
Ty du skall icke låta mina själ uti helvete; och icke tillstädja, att din Helige ser förgängelse. (Sheol h7585)
11 Inu mwandidziwitsa njira ya moyo; mudzandidzaza ndi chimwemwe pamaso panu, ndidzasangalala mpaka muyaya pa dzanja lanu lamanja.
Du kungör mig vägen till lifvet; för dig är glädje tillfyllest, och lustigt väsende på dine högra hand evinnerliga.

< Masalimo 16 >