< Masalimo 16 >
1 Mikitamu ya Davide. Ndisungeni Inu Mulungu, pakuti ine ndimathawira kwa Inu.
Varuj me, oh Bog, kajti vate polagam svoje trdno upanje.
2 Ndinati kwa Yehova, “Inu ndinu Ambuye anga; popanda Inu, ine ndilibe chinthu chinanso chabwino.”
O moja duša, Gospodu si rekla: »Ti si moj Gospod. Moja dobrota se ne razteza do tebe,
3 Kunena za oyera mtima amene ali pa dziko, amenewa ndi olemekezeka, amene ndimakondwera nawo.
temveč k svetim, ki so na zemlji in k odličnim, v katerih je vse moje zadovoljstvo.«
4 Anthu amene amathamangira kwa milungu ina mavuto awo adzachulukadi. Ine sindidzathira nawo nsembe zawo zamagazi kapena kutchula mayina awo ndi pakamwa panga.
Njihove bridkosti se bodo pomnožile, ki hitijo za drugim bogom. Njihovih krvavih pitnih daritev ne bom daroval niti njihovih imen ne bom jemal na svoje ustnice.
5 Yehova, Inu mwandipatsa cholowa changa ndi chikho changa; mwateteza kolimba gawo langa.
Gospod je delež moje dediščine in moje skodelice. Ti ohranjaš mojo usodo.
6 Malire a malo anga akhala pabwino; ndithudi, ine ndili cholowa chokondweretsa kwambiri.
Vrvice so mi padle na prijetnih krajih; da, lepo dediščino imam.
7 Ine ndidzatamanda Yehova amene amandipatsa uphungu; ngakhale usiku mtima wanga umandilangiza.
Blagoslavljal bom Gospoda, ki mi je dal nasvet. Moja notranjost me prav tako poučuje v nočnih obdobjih.
8 Ndayika Yehova patsogolo panga nthawi zonse. Popeza Iyeyo ali kudzanja langa lamanja, sindidzagwedezeka.
Vedno sem pred seboj postavljal Gospoda; ker je pri moji desnici, ne bom omajan.
9 Choncho mtima wanga ndi wosangalala ndipo pakamwa panga pakukondwera; thupi langanso lidzakhala pabwino,
Zato je moje srce veselo in moja slava se razveseljuje; tudi moje meso bo počivalo v upanju.
10 chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. (Sheol )
Kajti moje duše ne boš pustil v peklu niti ne boš trpel, da bi tvoj Sveti videl trohnobo. (Sheol )
11 Inu mwandidziwitsa njira ya moyo; mudzandidzaza ndi chimwemwe pamaso panu, ndidzasangalala mpaka muyaya pa dzanja lanu lamanja.
Pokazal mi boš stezo življenja. V tvoji prisotnosti je polnost radosti, pri tvoji desnici so zadovoljstva na vékomaj.