< Masalimo 16 >
1 Mikitamu ya Davide. Ndisungeni Inu Mulungu, pakuti ine ndimathawira kwa Inu.
Dal Dávidtól. Őrizz engem, Örökkévaló, mert benned kerestem menedéket.
2 Ndinati kwa Yehova, “Inu ndinu Ambuye anga; popanda Inu, ine ndilibe chinthu chinanso chabwino.”
Mondtam az Örökkévalónak: Uram vagy, javam nincsen rajtad kívűl.
3 Kunena za oyera mtima amene ali pa dziko, amenewa ndi olemekezeka, amene ndimakondwera nawo.
A szenteknek pedig, kik az országban vannak, és a dicsőknek, kikben egész kedvem van:
4 Anthu amene amathamangira kwa milungu ina mavuto awo adzachulukadi. Ine sindidzathira nawo nsembe zawo zamagazi kapena kutchula mayina awo ndi pakamwa panga.
Sokasodnak azoknak fájdalmai, kik más isteneket cserélnek; nem ontom véres ontóáldozataikat és nem veszem neveiket ajkaimra.
5 Yehova, Inu mwandipatsa cholowa changa ndi chikho changa; mwateteza kolimba gawo langa.
Az Örökkévaló osztályomnak és serlegemnek része; te tartod az én sorsomat.
6 Malire a malo anga akhala pabwino; ndithudi, ine ndili cholowa chokondweretsa kwambiri.
A mérő kötelek kellemetes helyekre estek számomra; birtokom is kedves előttem.
7 Ine ndidzatamanda Yehova amene amandipatsa uphungu; ngakhale usiku mtima wanga umandilangiza.
Áldom az Örökkévalót, ki nekem tanácsot adott, éjszakákon is oktattak engem veséim.
8 Ndayika Yehova patsogolo panga nthawi zonse. Popeza Iyeyo ali kudzanja langa lamanja, sindidzagwedezeka.
Az Örökkévalót mindig magam előtt tartottam; mert jobbomon van, nem tántorgok.
9 Choncho mtima wanga ndi wosangalala ndipo pakamwa panga pakukondwera; thupi langanso lidzakhala pabwino,
Annak örült szívem, és vigad méltóságom; testem is bizton lakozik.
10 chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. (Sheol )
Mert nem hagyod lelkemet az alvilágra, nem engeded jámborodat vermet látnia. (Sheol )
11 Inu mwandidziwitsa njira ya moyo; mudzandidzaza ndi chimwemwe pamaso panu, ndidzasangalala mpaka muyaya pa dzanja lanu lamanja.
“Tudatod velem az élet ösvényét: örömök bősége van színed előtt, kellemetesség a te jobbodban mindétig!