< Masalimo 16 >

1 Mikitamu ya Davide. Ndisungeni Inu Mulungu, pakuti ine ndimathawira kwa Inu.
ADAJE yo, O Yuus: sa iya jago nae gaegue y inangococo.
2 Ndinati kwa Yehova, “Inu ndinu Ambuye anga; popanda Inu, ine ndilibe chinthu chinanso chabwino.”
Ylegmo, O antijo, as Jeova: jago Señotto: taya minaulegco yaguin taegüe guiya jago.
3 Kunena za oyera mtima amene ali pa dziko, amenewa ndi olemekezeka, amene ndimakondwera nawo.
Ya y mañantos ni mangaegue gui tano, sija manmagas ya todo y minalagojo gaegue guiya sija.
4 Anthu amene amathamangira kwa milungu ina mavuto awo adzachulukadi. Ine sindidzathira nawo nsembe zawo zamagazi kapena kutchula mayina awo ndi pakamwa panga.
Mumegae y piniteñija ni tumolaeca si Jeova pot otro Yuus: ti juofrese ni y inefreseñija na jâgâ, ni juchule y naanñija gui labiosso.
5 Yehova, Inu mwandipatsa cholowa changa ndi chikho changa; mwateteza kolimba gawo langa.
Si Jeova y patten ni y ineredajo, yan y basujo: jago mumantietiene y fottunajo.
6 Malire a malo anga akhala pabwino; ndithudi, ine ndili cholowa chokondweretsa kwambiri.
Ya, y fottunajo upodong gui lugat na magof: magajet na bonito na ineredajo.
7 Ine ndidzatamanda Yehova amene amandipatsa uphungu; ngakhale usiku mtima wanga umandilangiza.
Jubendise si Jeova, ni y japagat yo: ya an puenge nae jafananagüe yo y jinasoco gui san jalomjo.
8 Ndayika Yehova patsogolo panga nthawi zonse. Popeza Iyeyo ali kudzanja langa lamanja, sindidzagwedezeka.
Si Jeova jupolo gui menajo para siempre: sa yaguin gaegue güe gui agapajo, ti siña yo manacalamten.
9 Choncho mtima wanga ndi wosangalala ndipo pakamwa panga pakukondwera; thupi langanso lidzakhala pabwino,
Enao mina magof y corasonjo ya magof y inenrajo: locue y catneco sumaga seguro.
10 chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. (Sheol h7585)
Sa ti undingo y antijo gui naftan: ni unnae y santosmo para ulie y minitong. (Sheol h7585)
11 Inu mwandidziwitsa njira ya moyo; mudzandidzaza ndi chimwemwe pamaso panu, ndidzasangalala mpaka muyaya pa dzanja lanu lamanja.
Unnatungoyo ni y chalan y linâlâ: binilan minagof y gaegue gui menamo: ya y agapa na canaemo guaja minagof para siempre.

< Masalimo 16 >