< Masalimo 150 >
1 Tamandani Yehova. Tamandani Mulungu mʼmalo ake opatulika; mutamandeni ku thambo lake lamphamvu.
ヱホバをほめたたへよ その聖所にて神をほめたたへよ その能力のあらはるる穹蒼にて神をほめたたへよ
2 Mutamandeni chifukwa cha machitidwe ake amphamvu; mutamandeni chifukwa cha ukulu wake wopambana.
その大能のはたらきのゆゑをもて神をほめたたへよ その秀ておほいなることの故によりてヱホバをほめたたへよ
3 Mutamandeni poyimba malipenga, mutamandeni ndi pangwe ndi zeze.
ラッパの聲をもて神をほめたたへよ 筝と琴とをもて神をほめたたへよ
4 Mutamandeni ndi matambolini ndi kuvina, mutamandeni ndi zingwe ndi zitoliro.
つづみと蹈舞とをもて神をほめたたへよ 絃簫をもて神をほめたたへよ
5 Mutamandeni ndi ziwaya zolira za malipenga, mutamandeni ndi ziwaya zolira kwambiri.
音のたかき鐃鈸をもて神をほめたたへよ なりひびく鐃鈸をもて神をほめたたへよ
6 Chamoyo chilichonse chopuma chitamande Yehova. Tamandani Yehova.
氣息あるものは皆ヤハをほめたたふべし なんぢらヱホバをほめたたへよ