< Masalimo 150 >

1 Tamandani Yehova. Tamandani Mulungu mʼmalo ake opatulika; mutamandeni ku thambo lake lamphamvu.
Alléluia! Louez Dieu en son sanctuaire, louez-le dans le firmament, siège de sa force.
2 Mutamandeni chifukwa cha machitidwe ake amphamvu; mutamandeni chifukwa cha ukulu wake wopambana.
Louez-le pour sa puissance, louez-le pour son immense grandeur.
3 Mutamandeni poyimba malipenga, mutamandeni ndi pangwe ndi zeze.
Louez-le aux sons stridents du Chofar, louez-le avec le luth et la harpe.
4 Mutamandeni ndi matambolini ndi kuvina, mutamandeni ndi zingwe ndi zitoliro.
Louez-le avec le tambourin et les instruments de danse, louez-le avec les instruments à cordes et la flûte.
5 Mutamandeni ndi ziwaya zolira za malipenga, mutamandeni ndi ziwaya zolira kwambiri.
Louez-le avec les cymbales sonores, louez-le avec les cymbales retentissantes.
6 Chamoyo chilichonse chopuma chitamande Yehova. Tamandani Yehova.
Que tout ce qui respire loue le Seigneur! Alléluia!

< Masalimo 150 >